Luka 8
Akazi otumikira Yesu ndi cuma cao 1 Ndipo kunali, katapita kamphindi anayendayenda kumizinda ndi kumidzi, kulalikira ndi kuwauza U thenga Wabwino wa Ufumu wa Mulungu, ndi pamodzi naye khumi ndi…
Akazi otumikira Yesu ndi cuma cao 1 Ndipo kunali, katapita kamphindi anayendayenda kumizinda ndi kumidzi, kulalikira ndi kuwauza U thenga Wabwino wa Ufumu wa Mulungu, ndi pamodzi naye khumi ndi…
Yesu atuma ophunzira ace kukalalikira mau 1 Ndipo iye anaitana pamodzi khumi ndi awiriwo nawapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse, ndi zakuciritsa nthenda. 2 Ndipo anawatuma kukalalikira Ufumu wa…
Yesu atuma ophunzira makumi asanu ndi awiri 1 Zitatha izi Ambuye anaika ena makumi asanu ndi awiri, nawatuma iwo awiri awiri pamaso pace ku mudzi uli wonse, ndi malo ali…
Pemphero la Ambuye 1 Ndipo kunali, pakukhala iye pamalo pena ndi kupemphera, m’mene analeka, wina wa ophunzira ace anati kwa iye, Ambuye, tiphunzitseni ife kupemphera, monganso Yohane anaphunzitsa ophunzira ace….
Yesu awacenjeza za cinyengo 1 Pomwepo pamene anthu a zikwi zikwi a khamu anasonkhana pamodzi, kotero kuti anapondana, iye anayamba kunena kwa ophunzira ace poyamba, Tacenierani nokha ndi cotupitsa mikate…
Maphedwe a Agalileya, tsanfa la Siloamu 1 Ndipo anakhalako nthawi yomweyo, anthu ena amene anamuuza iye za Agalileya, amene Pilato anasanganiza mwazi wao ndi nsembe zao. 2 Ndipo iye anayankha…
Yesu aciritsa munthu wodwala mbulu 1 Ndipo panali pamene iye analowa m’nyumba ya mmodzi wa akuru a Afarisi tsiku la Sabat a, kukadya, iwo analikumzonda iye. 2 Ndipo onani, panali…
Fanizo la nkhosa yosokera 1 Koma amisonkho onse ndi anthu ocimwa analikumyandikira kudzamva iye. 2 Ndipo Afarisi ndi alembi anadandaula nati, Uyu alandira anthu ocimwa, nadya nao. 3 Koma anati…
Fanizo la kapitao wonyenga 1 Ndipo iye ananenanso kwa ophunzira ace, Panali munthu mwini cuma, anali ndi kapitao wace; ndipo ameneyu ananenezedwa kwa iye kuti alikumwaza cuma cace. 2 Ndipo…
Za zolakwitsa, ndi makhululukidwe, ndi mphamvu ya cikhulupiriro ndi kutumikira kwathu 1 Ndipo anati kwa ophunzira ace, Sikutheka kuti zolakwitsa zisadze; koma tsoka iye amene adza nazo. 2 Kukolowekedwa mwala…