Marko 4
Fanizo La wofesa 1 Ndipo anayambanso kuphunzitsa pambali pa nyanja, Ndipo anasonkhana kwa Iye khamu lalikurukuru, kotero kuti analowa Iye mungalawa, nakhala m’nyanja; ndipo khamu lonse linakhala pamtunda m’mbali mwa…
Fanizo La wofesa 1 Ndipo anayambanso kuphunzitsa pambali pa nyanja, Ndipo anasonkhana kwa Iye khamu lalikurukuru, kotero kuti analowa Iye mungalawa, nakhala m’nyanja; ndipo khamu lonse linakhala pamtunda m’mbali mwa…
Yesu aciritsa wogwidwa ndi mzimu wonyansa ku Gerasa 1 Ndipo anafika tsidya lina la nyanja, ku dziko la Agerasa, 2 Ndipo pameneadaturuka mungalawa, pomwepo anakomana naye munthu woturuka kumanda wa…
Apeputsa Yesu ku Nazarete 1 Ndipo Iye anaturuka kumeneko; nafika ku dziko la kwao; ndipo ophunzira ace anamtsata. 2 Ndipo pofika dzuwa la Sabata, anayamba kuphunzitsa m’sunagoge; ndipo ambiri anamva…
Miyambo ya makolo ao 1 Ndipo anasonkhana kwa Iye Afarisi, ndi alembi ena, akucokera ku Yerusalemu, 2 ndipo anaona kuti ophunzira ace ena anadya mkate ndi m’manja mwakuda, ndiwo osasamba….
Yesu acurukitsa mikate kaciwiri 1 Masiku ajawo pakukhalanso khamu lalikuru la anthu, ndipo analibe kanthu kakudya, iye anadziitanira ophunzira ace, nanena nao, 2 Ndimva nalo cifundo khamulo, cifukwa ali ndi…
Mawalitsidwe a Yesu paphiri 1 Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu. 2…
Asasiyane mwamuna ndi mkazi wace 1 Ndipo ananyamuka Iye kumeneko, nadza ku maiko a ku Yudeya ndi ku tsidya lija la Yordano; ndipo anasonkhananso kwa Iye makamu a anthu; ndipo…
Yesu alowa m’Yerusalemu alikukhala pa buru 1 Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, pa phiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ace, 2 nanena nao, Mukani,…
Fanizo La osungira munda 1 Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m’mafanizo. Munthu analima munda wamphesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina. 2…
Yesu aneneratu za masautso alinkudza 1 Ndipo pamene analikuturuka Iye m’Kacisi, mmodzi wa ophunzira ace ananena kwa Iye, Mphunzitsi, onani, miyala yotere ndi nyumba yotere. 2 Ndipo Yesu anati kwa…