Marko 4

Fanizo La wofesa 1 Ndipo anayambanso kuphunzitsa pambali pa nyanja, Ndipo anasonkhana kwa Iye khamu lalikurukuru, kotero kuti analowa Iye mungalawa, nakhala m’nyanja; ndipo khamu lonse linakhala pamtunda m’mbali mwa…

Marko 5

Yesu aciritsa wogwidwa ndi mzimu wonyansa ku Gerasa 1 Ndipo anafika tsidya lina la nyanja, ku dziko la Agerasa, 2 Ndipo pameneadaturuka mungalawa, pomwepo anakomana naye munthu woturuka kumanda wa…

Marko 6

Apeputsa Yesu ku Nazarete 1 Ndipo Iye anaturuka kumeneko; nafika ku dziko la kwao; ndipo ophunzira ace anamtsata. 2 Ndipo pofika dzuwa la Sabata, anayamba kuphunzitsa m’sunagoge; ndipo ambiri anamva…

Marko 7

Miyambo ya makolo ao 1 Ndipo anasonkhana kwa Iye Afarisi, ndi alembi ena, akucokera ku Yerusalemu, 2 ndipo anaona kuti ophunzira ace ena anadya mkate ndi m’manja mwakuda, ndiwo osasamba….

Marko 8

Yesu acurukitsa mikate kaciwiri 1 Masiku ajawo pakukhalanso khamu lalikuru la anthu, ndipo analibe kanthu kakudya, iye anadziitanira ophunzira ace, nanena nao, 2 Ndimva nalo cifundo khamulo, cifukwa ali ndi…

Marko 9

Mawalitsidwe a Yesu paphiri 1 Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu. 2…

Marko 10

Asasiyane mwamuna ndi mkazi wace 1 Ndipo ananyamuka Iye kumeneko, nadza ku maiko a ku Yudeya ndi ku tsidya lija la Yordano; ndipo anasonkhananso kwa Iye makamu a anthu; ndipo…

Marko 11

Yesu alowa m’Yerusalemu alikukhala pa buru 1 Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, pa phiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ace, 2 nanena nao, Mukani,…

Marko 12

Fanizo La osungira munda 1 Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m’mafanizo. Munthu analima munda wamphesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina. 2…

Marko 13

Yesu aneneratu za masautso alinkudza 1 Ndipo pamene analikuturuka Iye m’Kacisi, mmodzi wa ophunzira ace ananena kwa Iye, Mphunzitsi, onani, miyala yotere ndi nyumba yotere. 2 Ndipo Yesu anati kwa…