Hoseya 9

Cimo la Israyeli ndi zotsatira zace 1 Usakondwera, Israyeli, ndi kusekerera, ngati mitundu ya anthu; pakuti wacita cigololo kuleka Mulungu wako, wakonda mphotho ya cigololo pa dwale la tirigu liri…

Hoseya 10

1 Israyeli ndi mpesa wotambalala, wodzibalira wokha zipatso; monga umo zinacurukira zipatso zace, momwemo anacurukitsa maguwa a nsembe ace; monga mwa kukoma kwace kwa dziko lace anapanga zoimiritsa zokoma. 2…

Hoseya 11

Kusayamika kwa Israyeli; macenjezo ndi malonjezo 1 Pamene Israyeli anali mwana, ndinamkonda, ndinaitana mwana wanga ali m’Aigupto. 2 Monga anawaitana, momwemo anawacokera; anaphera nsembe Abaala, nafukizira mafano osema. 3 Koma…

Hoseya 12

Mlandu wa Yehova pa Israyeli ndi Yuda 1 Efraimu akudya mphepo, natsata mphepo ya kum’mawa; tsiku lonse acurukitsa mabodza ndi cipasuko, ndipo acita pangano ndi Asuri, natenga mafuta kumka nao…

Hoseya 13

Cimo la Israyeli ndi kulangidwa kwace 1 Pamene Bfraimu analankhula panali kunjenjemera; anadzikweza m’Israyeli; koma pamene anaparamula mwa Baala, anafa. 2 Ndipo tsopano aonjeza kucimwa, nadzipangira mafano oyenga a siliva…

Hoseya 14

Mulungu adandaulira Israyeli alape, nalonjeza kuwakhululukira 1 Israyeli, bwerera kumka kwa Yehova Mulungu wako; pakuti wagwa mwa mphulupulu yako. 2 Mukani nao mau, nimubwerere kwa Yehova; nenani kwa Iye, Cotsani…

Yoweli 1

Tsoka locokera ku dzombe ndi cirala 1 MAU a Yehova a kwa Yoeli mwana wa Petueli. 2 Imvani ici, akulu akulu inu, nimuchere khutu, inu nonse okhala m’dziko. Cacitika ici…

Yoweli 2

Cilango coopsa ca Mulungu 1 Muombe lipenga m’Ziyoni, nimupfuulitse m’phiri langa lopatulika; onse okhala m’dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lirinkudza, pakuti liyandikira; 2 tsiku la mdima, la mdima wandiweyani,…

Yoweli 3

Aneneratu za cilango ca Mulungu pa adani ace; Israyeli adzakonrekanso 1 Pakuti taonani, masiku awo, ndi nthawi iyo, pamene ndibwera nao andende a Yuda ndi a Yerusalemu, 2 ndidzasonkhanitsa amitundu…

Amosi 1

Cilango ca Mulungu pa amitundu ozinga Israyeli 1 MAU a Amosi, amene anali mwa oweta ng’ombe a ku Tekoa, ndiwo amene anawaona za Israyeli masiku a Uziya mfumu ya Yuda,…