Danieli 11

1 Ndipo ine, caka coyamba ca Dariyo Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa. 2 Ndipo tsopano ndikufotokozera coonadi. Taona, adzaukanso mafumu atatu m’Perisiya, ndi yacinai idzakhala yoletnera ndithu yoposa onsewo; ndipo…

Danieli 12

Nthawi ya cimariziro, mau otsekedwa 1 Ndipo nthawi yomweyi adzauka Mikaeli kalonga wamkuru wakutumikira ana a anthu amtundu wako; ndipo padzakhala nthawi ya masautso, siinakhala yotere kuyambira mtundu wa anthu…

Hoseya 1

Hoseya akwatira mkazi woipa kufanizira zoipa za Israyeli 1 MAU a Yehova amene anadza kwa Hoseya mwana wa Beeri masiku a Uziya, Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda, ndi…

Hoseya 2

1 Nenani kwa abale anu, Anthu anga, ndi kwa alongo anu, Wocitidwa-cifundo. 2 Mutsutsane naye mai wanu, mutsutsane naye; pakuti sali mkazi wanga, ndi Ine sindiri mwamuna wace; ndipo acotse…

Hoseya 3

Akwatiranso mkazi woipa, kufaniziranso zocita ana a Israyeli 1 Ndipo Yehova anati kwa ine, Mukanso, konda mkazi wokondedwa ndi bwenzi lace, koma wakucita cigololo monga Yehova akonda ana a Israyeli,…

Hoseya 4

Mlandu pakati pa Mulungu ndi Israyeli 1 Imvani mau a Yehova, inu ana a Israyeli; pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi okhala m’dziko, popeza palibe coonadi, kapena cifundo, kapena kudziwa…

Hoseya 5

Kulowerera kwa Israyeli 1 Imvani ici, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israyeli; cherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti ciweruzoci cinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde…

Hoseya 6

Israyeli abwerera kunka kwa Yehova 1 Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang’amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga. 2 Atapita masiku awiri adzatitsitsimutsa, tsiku lacitatu adzatiutsa; ndipo tidzakhala ndi moyo pamaso pace….

Hoseya 7

Kucimwa ndi kupandukira kwa Israyeli 1 M’mene ndiciritsa Israyeli, mphulupulu ya Efraimu ibvumbuluka, ndi zoipa za Samariya; pakuti acita bodza, ndipo mkhungu alowa m’nyumba, ndi gulu la mbala manca kubwalo….

Hoseya 8

Kupembedza mafano ndi kusamvera kwa Israyeli 1 Lipenga kukamwa kwako, Akudza ngati ciombankhanga, kulim bana ndi nyumba ya Yehova; cifukwa analakwira cipangano canga, napikisana naco cilamulo canga. 2 Adzapfuulira kwa…