Yeremiya 26
Yeremiya aneneratu za kupasuka kwa Kacisi ndi Yerusalemu. Atsutsidwapo afe 1 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda, panadza mau awa ocokera kwa Yehova, kuti, 2…
Yeremiya aneneratu za kupasuka kwa Kacisi ndi Yerusalemu. Atsutsidwapo afe 1 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda, panadza mau awa ocokera kwa Yehova, kuti, 2…
Yeremiya awacenjeza agonje kwa mfumu ya ku Babulo 1 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda, mau awa anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, kuti, 2…
Yeremiya atsutsana ndi mneneri wonyenga, Hananiya 1 Ndipo panali caka comweco, poyamba Zedekiya kukhala mfumu ya Yuda, caka cacinai, mwezi wacisanu, kuti Hananiya mwana wa Azuri mneneri, amene anali wa…
Kalata wa Yeremiya wolembera kwa Ayuda otengedwa kunka ku Babulo 1 Amenewa ndi mau a kalata uja anatumiza Yeremiya mneneri kucokera ku Yerusalemu kunka kwa akuru otsala a m’nsinga, ndi…
Yehova alonjeza kubweza undende wa anthu a Israyeli 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, kuti, 2 Atero Yehova, Mulungu wa Israyeli, kuti, Lemba m’buku mau onse amene…
Mwa cikondi ca Mulungu adzabweza Israyeli 1 Nthawi yomweyo, ati Yehova, ndidzakhala Mulungu wa mabanja onse a Israyeli, ndipo iwo adzakhala anthu anga. 2 Atero Yehova, Anthu opulumuka m’lupanga anapeza…
Yeremiya atsekeredwa m’kaidi nagula munda wa Hanameli 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova caka cakhumi ca Zedekiya mfumu ya Yuda, cimene cinali caka cakhumi ndi cisanu ndi…
Yehova abwereza kunena kuti anthu ace adzakhazikikanso m’dziko mwao, padzakhalanso mphukira 1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yeremiya nthawi yaciwiri, pamene iye anali citsekedwere m’bwalo la kaidi, kuti, 2…
Zedekiya adzatengedwa, Yerusalemu adzalandidwa 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, pamene Nebukadinezara mfumu ya Babulo, ndi nkhondo yace yonse, ndi maufumu onse a dziko lapansi amene anagwira…
Kukhulupirika kwa Arekabu kukhale citsanzo ca kwa Yuda 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova masiku a Yehoyakimu mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda, kuti, 2 Pita ku…