Yeremiya 6

Acenjezedwa kuti adani adzamangira Yerusalemu misasa 1 Ananu a Benjamini, pulumukani pothawa pakati pa Yerusalemu, ombani lipenga m’Tekoa, kwezani cizindikiro m’Beti-hakeremu; pakuti caoneka coipa coturuka m’mpoto ndi kuononga kwakukulu. 2…

Yeremiya 7

Mneneri alikuima pa cipata ca Kacisi, achula mau akulonieza ndi akuopsa 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, kuti, 2 Ima m’cipata ca nyumba ya Yehova, lalikira m’menemo…

Yeremiya 8

1 Nthawi yomweyo, ati Yehova, adzaturutsa m’manda mwao mafupa a mafumu a Yuda, ndi mafupa a akuru ace, ndi mafupa a ansembe, ndi mafupa a aneneri, ndi mafupa a okhala…

Yeremiya 9

1 Ha, mutu wanga ukadakhala madzi, ndi maso anga kasupe wa misozi, kuti usana ndi usiku ndilirire ophedwa a mwana wamkazi wa anthu anga! 2 Ha, ndikadakhala ndi cigono ca…

Yeremiya 10

Mofano ndi acabe, Yehova ndiye 1 Tamvani mau amene Yehova anena kwa inu, nyumba ya Israyeli; 2 atero Yehova, a Musaphunzire njira ya amitundu, musaope zizindikiro za m’thambo; pakuti amitundu…

Yeremiya 11

Za kutyola panganolo 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, kuti, 2 Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu; 3 ndi…

Yeremiya 12

1 Wolungama ndinu, Yehova, pamene nditsutsana nanu mlandu; pokhapo ndinenane nanu za maweruzo; cifukwa canji ipindula njira ya oipa? cifukwa canji akhala bwino onyengetsa? 2 Inu mwabzyala iwo, inde, anagwiritsatu…

Yeremiya 13

Fanizo la mpango wabafuta lifanizira kulangidwa kwao 1 Atero Yehova kwa ine, Pita, udzigulire mpango wabafuta, nudzimangire m’cuuno mwako, usauike m’madzi. 2 Ndipo ndinagula mpango monga mwa mau a Yehova,…

Yeremiya 14

Yeremiya apempherera anthu 1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya onena za cirala. 2 Yuda alira, ndipo zipata zace zilefuka, zikhala pansi zobvekedwa ndi zakuda; mpfuu wa Yerusalemu wakwera….

Yeremiya 15

Yehova akanadi kumvera 1 Ndipo Yehova anati kwa ine, Ngakhale Mose ndi Samueli akadaima pamaso panga, koma mtima wanga sukadasamalira anthu awa; muwacotse iwo pamaso panga, aturuke. 2 Ndipo padzakhala,…