Yesaya 62
Cikhalidwe cokoma ca Yerusalemu 1 Cifukwa ca Ziyoni sindidzakhala cete, ndi cifukwa ca Yerusalemu sindidzapuma, kufikira cilungamo cace cidzaturuka monga kuyera, ndi cipulumutso cace monga nyali yoyaka. 2 Ndipo amitundu…
Cikhalidwe cokoma ca Yerusalemu 1 Cifukwa ca Ziyoni sindidzakhala cete, ndi cifukwa ca Yerusalemu sindidzapuma, kufikira cilungamo cace cidzaturuka monga kuyera, ndi cipulumutso cace monga nyali yoyaka. 2 Ndipo amitundu…
Mulungu adzapulumutsa anthu ace, nadzabwezera cilango owasautsa 1 Ndani uyu alinkudza kucokera ku Edomu, ndi zobvala zonika zocokera ku Bozira? uyu wolemekezeka m’cobvala cace, nayenda mu ukuru wa mphamvu zace?…
1 Mwenzi mutang’amba kumwamba ndi kutsikira pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu; 2 monga pamene moto uyatsa zitsamba, ndi moto uwiritsa madzi; kudziwitsa kwa amaliwongo anu dzina lanu, kuti amitundu…
Acenjeza osamvera kuti adzalangidwa 1 Iwo amene sanafunsa za Ine andifunafuna; ndi iwo amene sanandipwaira andipeza; ndinati, Taonani Ine, taonani Ine, kwa mtundu umene sunachula dzina langa. 2 Ndatambasulira manja…
Ocita zoipa adzabwezedwa cilango 1 Atero Yehova, Kumwamba ndi mpando wanga wacifumu, ndi dziko lapansi ndi coikapo mapazi anga; mudzandimangira Ine nyumba yotani? ndi malo ondiyenera kupumamo ali kuti? 2…
Kuitanidwa kwa Yeremiya akhale mneneri 1 MAU a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m’dziko la Benjamini; 2 amene anamdzera mau a Yehova masiku a Yosiya…
Yehova adzudzula anthu a lsrayeli 1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati, 2 Pita nupfuule n’makutu a Yerusalemu, kuti, Yehova atero, Ndikumbukira za iwe kukoma mtima kwa ubwana…
1 Amati, Ngati mwamuna acotsa mkazi wace, ndipo amcokera iye, nakhala mkazi wa wina, kodi adzabweranso kwa mkaziyo? dzikolo kodi silidzaipitsidwa? Koma iwe wacita dama ndi mabwenzi ambiri; koma bweranso…
1 Ngati udzabwera, Israyeli, ati Yehova, udzabwera kwa Ine; ndipo ngati udzacotsa zonyansa zako pamaso panga sudzacotsedwa. 2 Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m’zoonadi, m’ciweruziro, ndi m’cilungamo; ndipo mitundu ya anthu…
Malango a Mulungu pa Ayuda cifukwa ca zoipa zao zonse 1 Thamangani inu kwina ndi kwina m’miseu ya Yerusalemu, taonanitu, dziwani, ndi kufunafuna m’mabwalo ace, kapena mukapeza munthu, kapena alipo…