Mlaliki 12
1 Ukumbukirenso Mlengi wako masiku a unyamata wako, asanadze masiku oipa, ngakhale zisanayandikire zakazo zakuti udzati, Sindikondwera nazo; 2 ngakhale lisanade dzuwa, ndi kuunika, ndi mwezi, ndi nyenyezi, mitambo ndi…
1 Ukumbukirenso Mlengi wako masiku a unyamata wako, asanadze masiku oipa, ngakhale zisanayandikire zakazo zakuti udzati, Sindikondwera nazo; 2 ngakhale lisanade dzuwa, ndi kuunika, ndi mwezi, ndi nyenyezi, mitambo ndi…
Mkwatibwi anena ndi ana a Yerusalemu za mkwati 1 NYIMBO yoposa, ndiyo ya Solomo. 2 Mnyamatayo andipsompsonetse ndi m’kamwa mwace; Pakuti cikondi cako ciposa vinyo. 3 Mafuta ako anunkhira bwino;…
1 Ndine duwa lofiira la ku Saroni, Ngakhale kakombo wa kuzigwa. 2 Ngati kakombo pakati pa minga Momwemo wokondedwa wanga pakati pa ana akazi. 3 Ngati maula pakati pa mitengo…
Mkwatibwi apeza mkwati 1 Usiku pamphasa panga ndinamfunafuna amene moyo wanga umkonda: Ndinamfunafuna, koma osampeza. 2 Ndinati, Ndiuketu, ndiyendeyende m’mudzi, M’makwalala ndi m’mabwalo ace, Ndimfunefune amene moyo wanga umkonda: Ndimfunafuna,…
Mkwati alemekeza mkwatibwi 1 Taona, wakongola, bwenzi langa, namwaliwe, taona, wakongola; Maso ako akunga a nkhunda patseri pa cophimba cako: Tsitsi lako likunga gulu la mbuzi, Zooneka pa phiri la…
1 Ndalowa m’munda mwanga, mlongwanga, mkwatibwi: Ndachera nipa yanga ndi zonunkhiritsa zanga; Ndadya uci wanga ndi cisa cace; Ndamwa vinyo wanga ndi mkaka wanga. Idyani, atsamwalinu, Imwani, mwetsani cikondi. Alekana…
1 Bwenzi lako wapita kuti, Mkaziwe woposa kukongola? Bwenzi lako wapambukira kuti, Tikamfunefune pamodzi nawe? 2 Bwenzi langa watsikira kumunda kwace, Ku zitipula za mphoka, Kukadya kumunda kwace, ndi kuchera…
1 Ha, mapazi ako akongola m’zikwakwata, Mwana wamkaziwe wa mfumu! Pozinga m’cuuno mwako pakunga zonyezimira, Nchito ya manja a mmisiri waluso. 2 Pamcombo pako pakunga cikho coulungika, Cosasowamo vinyo wosanganika:…
1 Mwenzi utakhala ngati mlongwanga, Woyamwa pa bere la amai! Ndikadakupeza panja, ndikadakupsompsona; Osandinyoza munthu. 2 Ndikadakutsogolera, kukulowetsa m’nyumba ya amai, Kuti andilange mwambo; Ndikadakumwetsa vinyo wokoleretsa, Ndi madzi a…
Macimo ndi masauko a ana a lsrayeli 1 MASOMPHENYA a Yesaya mwana wa Amozi, amene iye anaona, onena za Yuda ndi Yerusalemu, masiku a Uziya, Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu…