Mlaliki 2
Za m’moyo uno sizitha kukondweretsa mtima 1 Ndinati mumtima mwanga, Tiyetu, ndikuyese ndi cimwemwe; tapenya tsono zabwino; ndipo taona, icinso ndi cabe. 2 Ndinati, Kuseka ndi misala; ndi cimwemwe kodi…
Za m’moyo uno sizitha kukondweretsa mtima 1 Ndinati mumtima mwanga, Tiyetu, ndikuyese ndi cimwemwe; tapenya tsono zabwino; ndipo taona, icinso ndi cabe. 2 Ndinati, Kuseka ndi misala; ndi cimwemwe kodi…
Ziri zofise ziri ndi nyengo yace, Mulungu ndi kuziika zonse 1 Kanthu kali konse kali ndi nthawi yace ndi cofuna ciri conse ca pansi pa thambo ciri ndi mphindi yace;…
Matsoka ndi mabvuto a moyo uno 1 Ndinabweranso tsono ndi kupenyera nsautso zonse zimacitidwa kunja kuno; ndipo taona, misozi ya otsenderezedwa, koma analibe wakuwatonthoza; ndipo akuwatsendereza anali ndi mphamvu koma…
Malangizo osiyana akuwasamalira anthu m’moyo uno 1 Samalira phazi lako popita ku nyumba ya Mulungu; pakuti kuyandikira kumvera kupambana kupereka nsembe za zitsiru; pakuti sizizindikira kuti zirikucimwa. 2 Usalankhule mwanthuku…
Ngakhale Mulungu apatsa munthu zonse azikhumba koma mtima sukhuta nazo 1 Pali coipa ndaciona kunja kuno cifalikira mwa anthu, 2 munthu amene Mulungu wamlemeretsa nampatsa cuma ndi ulemu, mtima wace…
Kumva zowawa nkokoma, nzeru ndi kudziletsa momwemo 1 Mbiri yabwino iposa zonunkhira zabwino; ndi tsiku lakumwalira liposa tsiku lakubadwa. 2 Kunka ku nyumba ya maliro kupambana kunka ku nyumba ya…
Langizo la kumvera mfumu 1 Ndani akunga wanzeru? Ndani adziwa tanthauzo la mau? Nzeru ya munthu iwalitsa nkhope yace, kuduwa kwa nkhope yace ndi kusanduka. 2 Nditi, Sunga mau a…
Okoma ndi oipa amamva zomwezo. Khalani nazo zakupatsa Mulungu mokondwera 1 Pakuti zonsezi ndinazisunga mumtima ndikalondoletu zonsezi; kuti olungama ndi anzeru ndi nchito zao ali m’manja a Mulungu; ngakhale kukonda…
Kupusa kusautsa kwambiri 1 Nchenche zakufa zinunkhitsa moipa nizioletsa mafuta onunkhira a sing’anga; comweco kupusa kwapang’ono kuipitsa iye amene achuka cifukwa ca nzeru ndi ulemu. 2 Wanzeru, mtima wace uli…
Tizicita zokoma lero lino posadziwa za mawa 1 Ponya zakudya zako pamadzi; udzazipeza popita masiku ambiri. 2 Gawira asanu ndi awiri ngakhale asanu ndi atatu; pakuti sudziwa coipa canji cidzaoneka…