Masalmo 83
Amitundu apangana kuononga Aisrayeli, Apempha Mulungu awalanditse Nyimbo. Satmo la Asatu. 1 Mulungu musakhale cete; Musakhale du, osanena kanthu, Mulungu. 2 Pakuti taonani, adani anu aphokosera: Ndipo okwiyira Inu aweramutsa…
Amitundu apangana kuononga Aisrayeli, Apempha Mulungu awalanditse Nyimbo. Satmo la Asatu. 1 Mulungu musakhale cete; Musakhale du, osanena kanthu, Mulungu. 2 Pakuti taonani, adani anu aphokosera: Ndipo okwiyira Inu aweramutsa…
Okhala m’nyumba ya Yehova ndiwo amwai Kwa Mkulu wa Nyimbo, pa Gitili: Salmo la ana a Kora. 1 Pokhala Inu mpotikonda ndithu, Yehova wa makamu! 2 Moyo wanga ulakalaka, inde…
Akumbutsa Mulungu madalitso akale, apempha awabwereze Kwa Mkulu wa Nyimbo: Satmo la ana a Kora. 1 Munacita zobvomereza dziko lanu, Yehova; Munabweza ukapolo wa Yakobo. 2 Munacotsa mphulupulu ya anthu…
Davide apempha Mulungu kolimba amlanditse Pemphero la Davide. 1 Cherani khutu lanu Yehova, mundiyankhe; Pakuti ine ndine wozunzika ndi waumphawi. 2 Sungani moyo wanga pakuti ine ndine wokondedwa wanu; Inu…
Yehova akonda Ziyoni Salmo la ana a Kora: Nyimbo. 1 Maziko ace ali m’mapiri oyera. 2 Yehova akonda zipata za Ziyoni Koposa zokhalamo zonse za Yakobo. 3 Mudzi wa Mulungu,…
Wa Salmo achula masautso ace, napempha Mulungu amdalitse kuimfa Nyimbo. Salmo la ana a Kora. Kwa Mkulu wa Nyimbo, pa Mahalata Leanotu. Cilangizo ca Hemana M-ezara. 1 Yehova, Mulungu wa…
Pangano la Mulungu ndi Davide. Mulungu adzapulumutsa anthu ace Cilangizo ca Etana M-ezera. 1 Ndidzayimbira zacifundo za Yehova nthawi yonse: Pakamwa panga ndidzadziwitsira cikhulupiriko canu ku mibadwo mibadwo. 2 Pakuti…
Mulungu ndiye wacikhalire, munthu ndiye wakutha msanga Pemphero la Mose munthu wa Mulungu. 1 Ambuye, Inu munatikhalira mokhalamo M’mibadwo mibadwo. 2 Asanabadwe mapiri, Kapena musanalenge dziko lapansi, ndi lokhalamo anthu,…
Mulungu asungadi wodzipereka kwa Iye 1 Iye amene akhala pansi m’ngaka yace ya Wam’mwambamwamba Adzagonera mu mthunzi wa Wamphamvuyonse. 2 Ndidzati kwa Yehova, Pothawirapo panga ndi linga langa; Mulungu wanga,…
Anthu onse ayamike Mulungu cifukwa ca nchito zace, cilungamo cace, ndi cifundo cace Satmo, Nyimbo ya pa Sabata, 1 Nkokoma kuyamika Yehova, Ndi kuyimbira nyimbo dzina lanu, Wam’mwambamwamba Inu: 2…