Yobu 35
Elihu akuti kwa Mulungu kulibe cifukwa ca kucita tsankhu 1 Ndipo Elihu anabwereza kunena, nati, 2 Kodi muciyesa coyenera, Umo mukuti, Cilungamo canga ciposa ca Mulungu, 3 Pakuti munena, Upindulanji…
Elihu akuti kwa Mulungu kulibe cifukwa ca kucita tsankhu 1 Ndipo Elihu anabwereza kunena, nati, 2 Kodi muciyesa coyenera, Umo mukuti, Cilungamo canga ciposa ca Mulungu, 3 Pakuti munena, Upindulanji…
Elihu alemekeza cilungamo ndi mphamvu ya Mulungu. Mulungu ndi wangwiro, ife tilephera kumdziwa 1 Elihu nabwereza, nati, 2 Mundilole pang’ono, ndidzakuuzani, Pakuti ndiri naonso mau akunenera Mulungu. 3 Ndidzatenga nzeru…
1 Pa icinso mtima wanga unienjemera, Nusunthika m’malo mwace. 2 Mvetsetsani cibumo ca mau ace, Ndi kugunda koturuka m’kamwa mwace. 3 Akumveketsa pansi pa thambo ponse, Nang’anipitsa mphezi yace ku…
Mulungu aonekera kwa Yobu osamtsutsa. Koma amkumbutsa za ukuru wopambana wa Mulungu. Yobu adzicepetsapo 1 Pamenepo Yehova anayankha Yobu m’kabvumvulu, nati, 2 Ndani uyu adetsa uphungu, Ndi mau opanda nzeru?…
1 Kodi udziwa nyengo yakuswana zinkhoma? Kodi wapenyerera pakuswa nswala? 2 Ukhoza kodi kuwerenga miyezi yakuzipitira, Kapena udziwa nyengo yoti ziswane? 3 Zithuntha, ziswa, Zitaya zowawa zao. 4 Ana ao…
1 Ndipo Yehova anabwereza kwa Yobu, nati, 2 Kodi wodzudzulayo atsutsane ndi Wamphamvuyonse? Wocita makani ndi Mulungu ayankhe. 3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova, nati, 4 Taonani, ndakhululuka ine, ndidzakubwezerani mau…
1 Kodi ukhoza kukoka ng’ona ndi mbedza? Kapena kukanikiza kalandira wace ndi cingwe? 2 Kodi ukhoza kumanga m’mphuno ndi mlulu? Kapena kuboola nsagwada wace ndi momba? 3 Kodi idzacurukitsa mau…
Yobu adzicepetsa pamaso pa Mulungu, mabwenziwo adzudzulidwa ndi Mulungu, Yobu apulumutsidwa nadalitsidwanso 1 Pamenepo Yobu anayankha Mulungu, nati, 2 Ndidziwa kuti mukhoza kucita zonse, Ndi kuti palibe coletsa colingirira canu…
Kusiyana pakati pa olungama ndi oipa 1 WODALA munthuyo wosayenda mu uphungu wa oipa, Kapena wosaimirira m’njira ya ocimwa, Kapena wosakhala pansi pa bwalo la onyoza. 2 Komatu m’cilamulo ca…
Ufumu wa wodzozedwa wa Yehova 1 Aphokoseranji amitundu. Nalingiriranji anthu zopanda pace? 2 Adzikhazikitsa mafumu a dziko lapansi, Nacita upo akulu pamodzi, Kutsutsana naye Yehova, ndi Wodzozedwa wace, ndi kuti….