Estere 5

Estere alowa kwa mfumu nampempha iye ndi Hamani azidya naye 1 Ndipo kunali tsiku lacitatu, Estere anabvala zobvala zace zacifumu, nakaimirira m’bwalo la m’kati la nyumba ya mfumu, popenyana pa…

Estere 6

Ahaswero aona cifukwa ca kucitira Moredekai ulemu 1 Usiku uja tulo tidamwazikira mfumu, niti abwere nalo buku la mbiri, naliwerenga pamaso pa mfumu. 2 Napeza mudalembedwa kuti Moredekai adaulula za…

Estere 7

Hamani aululidwa napacikidwa 1 Motero inadza mfumu ndi Hamani kumwa naye mkazi wamkuru Estere. 2 Nitinso mfumu kwa Estere tsiku laciwirili pa madyerero a vinyo, Pempho lanu nciani, mkazi wamkuru…

Estere 8

Ahaswero abvomereza pempho la Estere, Ayuda napulumuka 1 Tsiku lomwelo mfumu Ahaswero anampatsa mkazi wamkuru Estere nyumba ya Hamani mdani wa Ayuda, Nafika Moredekai pamaso pa mfumu; pakuti Estere adamuuza…

Estere 9

Ayuda awapha adani ao 1 Mwezi wakhumi ndi ciwiri tsono, ndiwo mwezi wa Adara, tsiku lace lakhumi ndi citatu, mau a mfumu ndi lamulo lace ali pafupi kucitika, tsikuli adani…

Estere 10

Ukuru wa Moredekai 1 Ndipo mfumu Ahaswero inasonkhetsa dziko, ndi zisumbu za ku nyanja yamcere. 2 Ndi zocita zonse za mphamvu yace, ndi nyonga zace, ndi mafotokozedwe a ukulu wa…

Yobu 1

Yobu wosautsidwabe alimbika kutama Mulungu 1 PANALI munthu m’dziko la Uzi, dzina lace ndiye Yobu; ndipo munthuyu anali wangwiro ndi woongoka, wakuopa Mulungu ndi kupewa zoipa. 2 Ndipo anabala ana…

Yobu 2

1 Panalinso tsiku lakuti anadza ana a Mulungu kudzionetsa kwa Yehova, nadza Satana yemwe pakati pao kudzionetsa kwa Yehova. 2 Ndipo Yehova anati kwa Satana, Ufuma kuti? Nayankha Satana, nati…

Yobu 3

Madandaulo a Yobu 1 Atatero, Yobu anatsegula pakamwa pace, natemberera tsiku lace. 2 Nalankhula Yobu nati, 3 Litayike tsiku lobadwa ine, Ndi usikuwo udati, Waima naye mwana wamwamuna. 4 Tsiku…

Yobu 4

Elifazi adzudzula Yobu; tsoka la munthu licokera ku zoipa zace; Yobu alape 1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati, 2 Munthu akayesa kunena nawe mau, kodi udzamva nao cisoni?…