Ezara 8
Maina a opita ndi Ezara. Ulendo wao mpaka Yerusalemu 1 Ndipo akuru a nyumba za makolo ndi awa, ndi cibadwidwe ca iwo okwera nane limodzi kucokera ku Babulo, pokhala mfumu…
Maina a opita ndi Ezara. Ulendo wao mpaka Yerusalemu 1 Ndipo akuru a nyumba za makolo ndi awa, ndi cibadwidwe ca iwo okwera nane limodzi kucokera ku Babulo, pokhala mfumu…
Mwankhawa Ezara apempherera Ayuda okwatira acilendo kwa Mulunzu 1 Zitatha izi tsono anandiyandikira akalonga, ndi kuti, Anthu a Israyeli, ndi ansembe, ndi Alevi, sanadzilekanitsa ndi anthu a maikowa, kunena za…
Acotsedwa akazi acilendo 1 Pakupemphera Ezara tsono, ndi kuulula ndi kulira misozi, ndi kudzigwetsa pansi pakhomo pa nyumba ya Mulungu, udamsonkhanira mwa Israyeli msonkhano waukuru ndithu wa amuna, ndi akazi,…
Nehemiya apempherera ana a lsrayeli kwa Mulungu 1 MAU a Nehemiya mwana wa Hakaliya. Kunali tsono mwezi wa Kisilevi, caka ca makumi awiri, pokhala ine ku Susani ku nyumba ya…
Aritasasta alola Nehemiya akamange linga la Yerusalemu 1 Koma kunacitika mwezi wa Nisana, caka ca makumi awiri ca Aritasasta mfumu pokhala vinyo pamaso pace, ndinatenga vinyoyo ndi kuipatsa mfumu. Koma…
Mamangidwe a malinga ndi zipata za Yerusalemu 1 Pamenepo Eliasibu mkuru wa ansembe ananyamuka pamodzi ndi abale ace ansembe, namanga cipata cankhosa; anacipatula, naika zitseko zace, inde anacipatula mpaka nsanja…
Adani ayesa kuwaletsa kumanga malinga 1 Ndipo kunali, atamva Sanibalati kuti tinalikumanga lingali, kudamuipira, nakwiya kwakukuru, naseka Ayuda pwepwete. 2 Nanena iye pamaso pa abale ace ndi ankhondo a ku…
Nehemiya acinjiriza aumphawi opsinjika 1 Pamenepo panamveka kulira kwakukuru kwa anthu ndi akazi ao kudandaula pa abale ao Ayuda. 2 Popeza panali ena akuti, Ife, ana athu amuna ndi akazi,…
Adani ayesa kunyenga ndi kuopsa Nehemiya 1 Kunali tsono, atamva Sanibalati, ndi Tobiya, ndi Gesemu M-arabu, ndi adani athu otsala, kuti ndidatha kumanga lingali, posatsalaponso popasuka; (ngakhale pajapo sindinaika zitseko…
Alonda adikira Yerusalemu 1 Ndipo atatha kumanga linga, ndinaika zitseko, nakhazika odikira, ndi oyimbira, ndi Alevi; 2 ndipo ndinawapatsa mbale wanga Hanani, ndi Hananiya kazembe wa kuboma, ulamuliro wa pa…