2 Mbiri 24

Yoasi akonzanso Kacisi 1 Yoasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa ufumu wace, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mace ndiye Zibiya wa ku Beereseba. 2…

2 Mbiri 25

Amaziya agonjetsa Aedomu 1 Amaziya anali wa zaka makumi awiri mphambu zisanu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zinai; ndi dzina la mace ndiye…

2 Mbiri 26

Uziyaagonjetsa adani ambiri 1 Ndipo anthu onse Ayuda anatenga Uziya, ndiye wa zaka khumi mphambu zisanu ndi cimodzi, namlonga ufumu m’malo mwa atate wace Amaziya. 2 Iye anamanga Eloti, naubweza…

2 Mbiri 27

Yotamu mfumu ya Yuda 1 Yotamu anali wa zaka makumi awiri, mphambu zisanu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka khumi ndi zisanu ndi cimodzi; ndi dzina la mace ndiye…

2 Mbiri 28

Ahazi mfumu yoipitsitsa ya Yuda 1 Ahazi anali wa zaka makumi awiri polowa ufumu wace, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka khumi mphambu zisanu ndi cimodzi; koma sanacita zoongoka pamaso pa Yehova…

2 Mbiri 29

Hezekiya mfumu ya Yuda 1 Hezekiya analowa ufumu wace ali wa zaka makumi awiri mphambu zisanu, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zinai; ndi dzina la mace…

2 Mbiri 30

Hezekiya acita Paskha ku Yerusalemu 1 Ndipo Hezekiya anatumiza kwa Israyeli ndi Yuda onse, nalembanso akalata kwa Efraimu ndi Manase, kuti abwere ku nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, kucitira Yehova…

2 Mbiri 31

Afafaniza cipembedzo conse ca mafano 1 Citatha ici conse tsono, Aisrayeli onse opezekako anaturuka kumka ku midzi ya Yuda, naphwanya zoimiritsa, nalikha zifanizo, nagamula misanje ndi maguwa a nsembe m’Yuda…

2 Mbiri 32

Sanakeribu agwera Yuda 1 Zitatha zinthu izi zokhulupirika, anadza Sanakeribu mfumu ya Asuri, nalowera Yuda, namangira midzi yamalinga misasa, nati adzigonjetsere iyi. 2 Ndipo pakuona Hezekiya kuti wadza Sanakeribu, ndi…

2 Mbiri 33

Manase aikanso cipembedza ca mafano 1 Manase anali wa zaka khumi ndi ziwiri polowa ufumu wace, nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi asanu mphambu zisanu. 2 Nacita coipa pamaso pa Yehova,…