2 Mbiri 4
Guwa la nsembe ndi thawale lamkawa ndi zipangizo zonse zina 1 Anapanganso guwa la nsembe lamkuwa, m’litali mwace mikono makumi awiri, ndi kupingasa kwace mikono makumi awiri, ndi msinkhu wace…
Guwa la nsembe ndi thawale lamkawa ndi zipangizo zonse zina 1 Anapanganso guwa la nsembe lamkuwa, m’litali mwace mikono makumi awiri, ndi kupingasa kwace mikono makumi awiri, ndi msinkhu wace…
1 Momwemo zidatha nchito zonse Solomo adazicitira nyumba ya Yehova. Ndipo Solomo anabwera nazo zopatulika zija za atate wace Davide; naziika siliva, ndi golidi, ndi zipangizo zonse m’cuma ca nyumba…
Conena Solomo ndi pemphero lace popereka Kacisi 1 Pamenepo Solomo anati, Yehova anati kuti adzakhala mu mdima wandiweyani. 2 Koma ndakumangirani nyumba yokhalamo, malo okhazikika okhalamo Inu nthawi yosatha. 3…
Cibvomerezo ca Yehova mwa moto ndi ulemerero wao wodzaza Kacisi 1 Atatha tsono Solomo kupemphera, moto unatsika kumwamba, nunyeketsa nsembe yopsereza, ndi nsembe zophera; ndipo ulemerero wa Yehova unadzaza nyumbayi….
Solomo amanga midzi yina 1 Ndipo kunali, zitatha zaka makumi awiri m’mene anamanga nyumba ya Yehova, ndi nyumba yace yace, 2 Solomo anamanga midzi imene Huramu adampatsa, nakhalitsamo ana a…
Mfumu yaikazi ya ku Seba aceza ndi Solomo 1 Ndipo atamva mfumu yaikazi ya ku Seba mbiri ya Solomo, anadza kumuyesera Solomo ndi miyambi yododometsa ku Yerusalemu, ndi ulendo waukuru,…
Ufumu ugawanika pakati. Rehabiamu mfumu ya Yuda, Yerobiamu ya Israyeli 1 Ndipo Rehabiamu anamuka ku Sekemu; pakuti Aisrayeli onse adadza ku Sekemu kumlonga ufumu. 2 Ndipo kunali, atamva Yerobiamu mwana…
Mulungu aletsa nkhondo pakati pa Yuda ndi Israyeli 1 Ndipo atafika ku Yerusalemu Rehabiamu, anamemeza a nyumba ya Yuda ndi Benjamini amuna osankhika zikwi zana limodzi mphambu makumi asanu ndi…
Sisaki wa ku Aigupto athira nkhondo Rehabiamu 1 Ndipo kunacitika, utakhazikika ufumu wa Rehabiamu, nalimbika iye, anasiya cilamulo ca Yehova, ndi Aisrayeli onse pamodzi naye. 2 Ndipo Rehabiamu atakhala mfumu…
Abiya ndi Yerobiamu agwirana nkhondo, Israyeli akanthidwa 1 Ndipo caka cakhumi mphambu zisanu ndi zitatu ca Yerobiamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda. 2 Anakhala mfumu m’Yerusalemu zaka zitatu; ndi dzina…