2 Mafumu 18
Hezekiya wabwino akhazikanso cipembedzo ca Yehova 1 Ndipo kunali caka cacitatu ca Hoseya mwana wa Ela mfumu ya Israyeli, Hezekiya mwana wa Ahazi mfumu ya Yuda analowa ufumu waceo 2…
Hezekiya wabwino akhazikanso cipembedzo ca Yehova 1 Ndipo kunali caka cacitatu ca Hoseya mwana wa Ela mfumu ya Israyeli, Hezekiya mwana wa Ahazi mfumu ya Yuda analowa ufumu waceo 2…
Nkhawa ya Hezekiya ndi pemphero lace 1 Ndipo kunali, atamva Hezekiya, anang’amba zobvala zace, napfundira ciguduli, nalowa m’nyumba ya Yehova. 2 Natuma Eliyakimu woyang’anira nyumbayo, ndi Sebina mlembi, ndi akuru…
Hezekiya adwala nacira 1 Masiku ajawo Hezekiya anadwala, nafuna kufa. Namdzera Yesaya mneneri mwana wa Amozi, nanena naye, Atero Yehova, Siyira banja lako; pakuti udzafa, sudzakhala ndi moyo. 2 Pamenepo…
Manase woipitsitsa 1 Manase anali wa zaka khumi ndi ziwiri polowa iye ufumu wace, nakhala mfumu zaka makumi asanu ndi zisanu m’Yerusalemu; ndi dzina la mace ndiye Hefisiba. 2 Ndipo…
Yosiya wabwino akonzanso kacisi 1 Yosiya ndiye wa zaka zisanu ndi zitatu polowa ufumu wace, nakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu cimodzi m’Yerusalemu; ndi dzina la mace ndi Yedida mwana…
Yosiya awerenga bukulo kwa anthu nacita pangano ndi Yehova, nakonza zoipsa zambiri 1 Pamenepo mfumu inatumiza anthu, namsonkhanitsira akulu onse a Yuda ndi a m’Yerusalemu. 2 Nikwera mfumu kumka ku…
1 Masiku ace Nebukadinezara mfumu ya ku Babulo anakwerako, Yoyakimu nagwira mwendo wace zaka zitatu; pamenepo anatembenuka nampandukira. 2 Ndipo Yehova anamtumizira magulu a Akasidi, ndi magulu a Aaramu, ndi…
Yerusalemu apasulidwa, anthu natengedwa kunka ku Babulo 1 Ndipo kunali caka cacisanu ndi cinai ca ufumu wace, mwezi wakhumi, tsiku lakhumi la mwezi, Nebukadinezara mfumu ya Babulo, iye ndi khamu…
Maina a makolo kuyambira Adamu kufikira adzukulu a Nowa 1 ADAMU, Seti, Enosi, 2 Kenani, Mahalaheli, Yaredi, 3 Enoki, Metusela, Lameki, 4 Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti. 5 Ana a…
Ana a Israyeli, adzukulu a Yuda 1 Ana a Israyeli ndi awa: Rubeni, Simeoni, Levi, ndi Yuda, Isakara, ndi Zebuluni, 2 Dani, Yosefe, ndi Benjamini, Nafitali, Gadi, ndi Aseri. 3…