2 Mafumu 8
Wa ku Sunemu abwera kwao itatha njalayo 1 Ndipo Elisa ananena ndi mkazi uja adamuukitsira mwana wace, kuti, Nyamuka, numuke iwe ndi banja lako, nugonere komwe ukaone malo; pakuti Yehova…
Wa ku Sunemu abwera kwao itatha njalayo 1 Ndipo Elisa ananena ndi mkazi uja adamuukitsira mwana wace, kuti, Nyamuka, numuke iwe ndi banja lako, nugonere komwe ukaone malo; pakuti Yehova…
Yehu adzozedwa mfumu ya Israyeli 1 Ndipo Elisa mneneriyo anaitana mmodzi wa ana a aneneri, nanena naye, Udzimangire m’cuuno, nutenge nsupa iyi ya mafuta m’dzanja mwako, numuke ku Ramoti Gileadi….
Yehu aononga mbumba ya Ahabu 1 Ndipo Ahabu anali nao ana amuna makumi asanu ndi awiri m’Samariya. Nalemba akalata Yehu, natumiza ku Samariya kwa akulu a Yezreeli, ndiwo akulu akulu,…
A taliya aononga mbumba yacifumu ya Yuda; apulumuka Yoasi, aphedwa Ataliya 1 Pamene Ataliya mace wa Ahaziya anaona kuti mwana wace wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yacifumu. 2 Koma Yoseba…
Yoasi akonza Kacisi 1 Caka cacisanu ndi ciwiri ca Yehu, Yoasi analowa ufumu wace; nakhala mfumu m’Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mai wace ndiye Zibiya wa ku Beereseba….
Yoahazi mfumu ya Israyeli 1 Caka ca makumi awiri ndi zitatu ca Yoasi mwana wa Ahaziya mfumu ya Yuda, Yoahazimwana wa Yehu analowa ufumu wace wa Israyeli ku Samariya, nakhala…
Amaziyamfumu ya Yuda, Yoasi ndi Yerobiamu waciwiri mafumu a Israyeli 1 Caka caciwiri ca Yoasi mwana wa Yoahazi mfumu ya Israyeli, Amaziya mwana wa Yoasi mfumu ya Yuda analowa ufumu…
Azariya mfumu ya Yuda 1 Caka ca makumi awiri mphambu zisanu ndi ziwiri ca Yerobiamu mfumu ya Israyeli, Azariya mwana wa Amaziya mfumu ya Yuda analowa ufumu wace. 2 Anali…
Ahazi mfumu ya Yuda 1 Caka cakhumi mphambu zisanu ndi ziwiri ca Peka mwana wa Remaliya Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya Yuda analowa ufumu wace. 2 Ahazi anali wa…
Hoseyamfumu yotsiriza ya Israyeli, Salimanezeri mfumu ya Asuri apasula Samariya, Aisrayeli natengedwa ukapolo 1 Caka cakhumi ndi ziwiri ca Ahazi mfumu ya Yuda Hoseya mwana wa Ela analowa ufumu wace…