2 Samueli 14

Abisalomu abwera ku Yerusalemu 1 Ndipo Yoabu mwana wa Zeruya anazindikira kuti mtima wa mfumu unalunjika kwa Abisalomu. 2 Ndipo Yoabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye,…

2 Samueli 15

Kupanduka kwa Abisalomu, ndi kuthawa kwa Davide 1 Ndipo kunali, citapita ici Abisalomu anadzikonzera gareta ndi akavalo ndi anthu makumi asanu akuthamanga momtsogolera. 2 Ndipo Abisalomu analawirira, nakaima pa njira…

2 Samueli 16

Davide akomana ndi Ziba. Simeyi amtukwana 1 Ndipo pamene Davide anapitirira pang’ono pamutu pa phiri, onani, Ziba mnyamata wa Mefiboseti anakomana naye, ali nao aburu awiri omanga mbereko, ndi pamenepo…

2 Samueli 17

Ndipo Ahitofeli ananena ndi 1 Abisalomu, Ndiloleni ndisankhe tsopano anthu zikwi khumi ndi ziwiri, ndipo ndidzanyamuka usiku womwe uno ndi kulondola Davide; 2 ndipo ndidzamgwera ali wolema ndi wofoka, ndi…

2 Samueli 18

1 Ndipo Davide anawerenga anthu amene anali naye, nawaikira atsogoleri a zikwi ndi atsogoleri a mazana. 2 Davide natumiza anthu atawagawa magulu atatu, gulu limodzi aliyang’anire Yoabu, lina aliyang’anire Abisai,…

2 Samueli 19

Yoabu adzudzula Davide 1 Ndipo anauza Yoabu, Onani mfumu irikulira misozi, nilira Abisalomu. 2 Ndipo cipulumutso ca tsiku lila cinasandulika maliro kwa anthu onse; pakuti anthu anamva kuti, Mfumu iri…

2 Samueli 20

Mpanduko ndi imfa ya Seba 1 Ndipo kudangotero kuti pamenepo panali munthu woipa, dzina lace ndiye Seba mwana wa Bikri Mbenjamini; naliza iye lipenga, nati, Ife tiribe gawo mwa Davide,…

2 Samueli 21

Njala m’dziko, cifukwa cace, matsirizidwe ace 1 Ndipo m’masiku a Davide munali odala, zaka zitatu; ndipo Davide anafunsira kwa Yehova. Ndipo Yehova anati, Ndico cifukwa ca Sauli ndi nyumba yace…

2 Samueli 22

Nyimbo yoyamikira ya Davide 1 Ndipo Davide analankhula kwa Yehova mau a nyimbo iyi tsikuli Yehova anampulumutsa m’dzanja la adani ace onse, ndi m’dzanja la Sauli. 2 Ndipo anati:- Yehova…

2 Samueli 23

Nyimbo yotsiriza ya Davide 1 Ndipo mau otsiriza a Davide ndi awa:— Atero Davide mwana wa Jese, Atero munthu wokwezedwa, Ndiye wodzozedwa wa Mulungu wa Yakobo, Ndi mwini masalmo wokoma…