1 Samueli 25
Amwalira Samueli 1 Ndipo Samueli anamwalira; ndi Aisrayeli onse anaunjikana pamodzi nalira maliro ace, namuika m’nyumba yace ku Rama. Davide nanyamuka, natsikira ku cipululu ca Parana. Za Davide, Nabala ndi…
Amwalira Samueli 1 Ndipo Samueli anamwalira; ndi Aisrayeli onse anaunjikana pamodzi nalira maliro ace, namuika m’nyumba yace ku Rama. Davide nanyamuka, natsikira ku cipululu ca Parana. Za Davide, Nabala ndi…
Davide alekanso Sauli osamupha 1 Ndipo Azifi anafika kwa Sauli ku Gibeya, nati, Kodi Davide sali kubisala m’phiri la Hagila, kupenya kucipululu! 2 Ndipo Sauli ananyamuka, natsikira ku cipululu ca…
1 Ndipo Davide ananena mumtima mwace, Tsiku tina Sauli adzandipha; palibe cina condikomera koma kuti ndithawire ku dziko la Afilisti; ndipo Sauli adzakhala kakasi cifukwa ca ine, osandifunanso m’malire onse…
Sauli afunsira mkazi wobwebweta ku Endori 1 Ndipo kunali masiku aja, Afilisti anasonkhanitsa pamodzi makamu ao onse kunkhondo, kuti akaponyane ndi Aisrayeli. Ndipo Akisi ananena ndi Davide, Dziwa kuti zoonadi,…
Afilisti abweza Davide kunkhondo 1 Tsono Afilisti anasonkhanitsa makamu ao onse ku Afeki; ndipo Aisrayeli anamanga ku citsime ca m’Jezreeli. 2 Ndipo akalonga a Afilisti ananyamuka ndi mazana ao ndi…
Davide alanditsa a ku Zikilaga m’manja mwa Aamaleki 1 Ndipo kunali, pakufika Davide ndi anthu ace ku Zikilaga tsiku lacitatu, Aamaleki adaponya nkhondo yobvumbulukira kumwera, ndi ku Zikilaga, nathyola Zikilaga…
Sauli ndi ana ace atatu aphedwa ndi Afilisti pa Giliboa 1 Ndipo Afilisti anaponyana ndi Aisrayeli; Aisrayeli nathawa pamaso pa Afilisti, nagwa olasidwa m’phiri la Giliboa. 2 Ndipo Afilisti anapitikitsa,…
Amuuza Davide za imfa ya Sauli 1 NDIPO kunali atamwalira Sauli, pamene Davide anabwera atawapha Aamaleki, ndipo Davide atakhala ku Zikilaga masiku awiri; 2 pa tsiku lacitatu, onani, munthu anaturuka…
Davide alowa ufumu wa Yuda 1 Ndipo zitatha izi Davide anafunsira kwa Yehova nati, Kodi ndikwere kunka m’mudzi wina wa Yuda? Ndipo Yehova ananena naye, Kwera. Davide nanena naye, Ndikwere…
1 Ndipo panali nkhondo nthawi yaitali pakati pa nyumba ya Sauli ndi nyumba ya Davide. Koma Davide analimba cilimbire, ndi nyumba ya Sauli inafoka cifokere. Ana obadwira Davide ku Hebroni…