1 Samueli 5

Likasa la Mulungu ku nyumba ya Dagoni 1 Ndipo Afilisti anatenga likasa la Mulungu, nacoka nalo ku Ebenezeri, napita ku Asidodi. 2 Ndipo Afilistiwo anatenga likasa la Mulungu, nafika nalo…

1 Samueli 6

Afilisti abweza likasa ku dziko la Aisrayeli 1 Ndipo likasa la Yehova linakhala ku dziko la Afilisti miyezi isanu ndi iwiri. 2 Ndipo Afilistiwo anaitana ansembe ndi oombeza, nati, Ticitenji…

1 Samueli 7

1 Ndipo anthu a ku Kiriati-yearimu anabwera, natenga likasa la Yehova, nafika nalo m’nyumba ya Abinadabu paphiri; napatula mwana wace wamwamuna Eleazeri kuti asunge likasa la Yehova. Afilisti akanthidwa ku…

1 Samueli 8

Aisrayeli akhumba mfumu 1 Ndipo kunali, pamene Samueli anakalamba, anaika ana ace amuna akhale oweruza a Israyeli. 2 Dzina la mwana wace woyamba ndiye Yoeli, ndi dzina la waciwiri ndiye…

1 Samueli 9

Sauli afuna aburu olowerera a atate wace 1 Ndipo panali munthu Mbenlamlni, dzina lace ndiye Kisi, mwana wa Abiyeli, mwana wa Zerori, mwana wa Bekorati, mwana wa Afiya, mwana wa…

1 Samueli 10

Samueli; adzoza Sauli akhale mfumu ya Israyeli 1 Pamenepo Samueli anatenga nsupa ya mafuta, nawatsanulira pamutu pace, nampsompsona iye, nati, Sanakudzozani ndi Mulungu kodi, mukhale mfumu ya pa colowa cace?…

1 Samueli 11

Sauli alanditsa Yabezi Gileadi m’manja mwa Aamoni 1 Pamenepo Nahasi M-amoni anakwera, namanga Yabezi Gileadi zithando; ndipo anthu onse a ku Yabezi anati kwa Nahasi, Mupangane cipangano ndi ife, ndipo…

1 Samueli 12

Samueli adzinenera kwa anthu 1 Ndipo Samueli anauza Aisrayeli onse, kuti, Onani dani ndinamvera mau anu mwa zonse munalankhula ndi ine, ndipo ndinakulongerani mfumu. 2 Ndipo tsopano, siyi mfumu idzayendabe…

1 Samueli 13

Nkhondo pakati pa Israyeli ndi Afilisti 1 Sauli anali ndi zaka makumi atatu pamene anayamba ufumu wace; nakhala mfumu ya Israyeli zaka ziwiri. 2 Pamenepo Sauli anadzisankhira anthu zikwi zitatu…

1 Samueli 14

Jonatani agonjetsa Afilisti 1 Ndipo kunali tsiku lina kuti Jonatani mwana wa Sauli ananena ndi mnyamata wonyamula zida zace, Tiye tipite kunka ku kaboma ka Afilisti, tsidya lija. Koma sanauza…