Oweruza 20
Aisrayeli abwezera cilango pfuko la Benjamini 1 Pamenepo anaturuka ana onse a Israyeli, nuunjikana msonkhano kwa Yehova ku Mizipa ngati munthu mmodzi, kuyambira ku Dani mpaka Beereseba ndi dziko la…
Aisrayeli abwezera cilango pfuko la Benjamini 1 Pamenepo anaturuka ana onse a Israyeli, nuunjikana msonkhano kwa Yehova ku Mizipa ngati munthu mmodzi, kuyambira ku Dani mpaka Beereseba ndi dziko la…
Pfuko la Benjamini limangidwanso 1 Koma amuna a Israyeli adalumbira ku Mizipa, ndi kuti, Palibe mmodzi wa ife adzapereka mwana wace wamkazi kwa Mbenjamini akhale mkazi wace. 2 Ndipo anthu…
Naomi ndi apongozi ace awiri 1 NDIPO masiku akuweruza oweruzawo munali njala m’dziko. Ndipo munthu wa ku Betelehemu-Yuda anamuka nakagonera m’dziko la Moabu, iyeyu, ndi mkazi wace, ndi ana ace…
Rute akunkha m’munda wa Boazi 1 Ndipo Naomi anali nave mbale wa mwamuna wace, ndiye munthu mwini cuma cambiri wa banja la Elimeleki; dzina lace ndiye Boazi. 2 Nati Rute…
Boazi anena za kumuombolera Rute colowa 1 Pamenepo Naomi mpongozi wace ananena naye, Mwana wanga, kodi ndisakufunire popumulako, kuti ukhale bwino? 2 Nanga Boazi wodziwana nafe, amene unakhala nao adzakazi…
Boazi akwatira Rute nabadwa Obedi 1 Ndipo Boazi anakwera kumka kucipata, nakhala pansi pomwepo; ndipo taona, woombolera winayo adanena Boazi analinkupita; nati iye, Iwe uje, pambuka, khala pansi apa; napambuka…
1 NDIPO panali munthu wina wa ku Ramatayimu Zofimu, wa dziko la mapiri la Efraimu, dzina lace ndiye Elikana, mwana wace wa Yerohamu, mwana wa Elihu, mwana wa Tohu, mwana…
Coyamikira ca Hana 1 Ndipo Hana anapemphera, nati Mtima wanga umyuka mokondwera kwa Yehova, Nyanga yanga yakwezeka mwa Yehova; Pakamwa panga pakula kwa adani anga; Popeza ndikondwera m’cipulumutsocanu. 2 Palibe…
Masomphenya a Samueli 1 Ndipo mwanayo Samueli anatumikira Yehova pamaso pa Eli. Ndipo masiku aja mau a Yehova anamveka kamodzi kamodzi; masomphenya sanaoneka-oneka. 2 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona…
Afilisti akantha Aisrayeli 1 Ndipo mau a Samueli anafikira kwa Aisrayeli onse. Ndipo Aisrayeli anaturuka kukaponyana nkhondo ndi Afilisti, namanga zithando zao ku Ebenezeri; Afilistiwo namanga m’Afeki. 2 Ndipo Afilistiwo…