Genesis 11
Nsanja ya Babele 1 Ndipo dziko lapansi linali la cinenedwe cimodzi ndi cilankhulidwe cimodzi. 2 Ndipo panali pamene anayendayenda ulendo kum’mawa, anapeza cigwa m’dziko la Sinara, ndipo anakhala kumeneko. 3…
Nsanja ya Babele 1 Ndipo dziko lapansi linali la cinenedwe cimodzi ndi cilankhulidwe cimodzi. 2 Ndipo panali pamene anayendayenda ulendo kum’mawa, anapeza cigwa m’dziko la Sinara, ndipo anakhala kumeneko. 3…
Kuitanidwa kwa Abramu 1 Ndipo Yehova anati kwa Abramu, Turuka iwe m’dziko lako, ndi kwa abale ako, ndi ku nyumba ya atate wako, kunka ku dziko limene ndidzakusonyeza iwe; 2…
Abramu ndi Loti alekana 1 Ndipo anakwera Abramu kucoka ku Aigupto, iye ndi mkazi wace, ndi zonse anali nazo, ndi Loti pamodzi naye, kunka ku dziko la kumwera. 2 Ndipo…
Abramu alanditsa Loti 1 Ndipo panali masiku a Amarafele mfumu ya Sinara, ndi Arioki mfumu ya Elasara, ndi Kedorelaomere mfumu ya Elami, ndi Tidala mfumu ya Goimu, 2 iwo anathira…
Mulungu apangana ndi Abramu 1 Zitapita izo, mau a Yehova anadza kwa Abramu m’masomphenya, kuti, Usaope, Abramu, Ine ndine cikopa cako ndi mphotho yako yaikurukuru. 2 Ndipo Abramu anati, Ambuye…
Sara ndi Hagara 1 Ndipo Sarai mkazi wace wa Abramu sanambalire iye mwana; ndipo anali ndi mdzakazi, wa ku Aigupto, dzina lace Hagara. 2 Ndipo Sarai anati kwa Abramu, Taonanitu,…
Dzina la Abramu lisinthika likhale Abrahamu 1 Pamene Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, Yehova anamuonekera Abramu nati kwa iye, Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse;…
Amithenga atatu amuonekera Abrahamu 1 Ndipo Yehova anamuonekera iye pa mtengo yathundu ya ku Mamre, pamene anakhala pa khomo la hema wace pakutentha dzuwa. 2 Ndipo anatukula maso ace, nayang’ana,…
Cionongeko ca Sodomu ndi Gomora 1 Ndipo anadza ku Sodomu madzulo amithenga awiri; ndipo Loti anakhala pa cipata ca Sodomu, ndipo Loti anaona iwo, nauka kuti akakomane nao, ndipo anaweramitsa…
Abrahamu kwa mfumu Abimeleke 1 Abrahamu ndipo anacoka kumeneko kunka ku dziko la kumwera, ndipo anakhala pakati pa Kedesi ndi Suri, ndipo anakhala ngati mlendo m’Gerari. 2 Ndipo Abrahamu anati…