Deuteronomo 8
Akumbuke zokoma zazikuru Mulungu anawacitira 1 Muzisamalira kucita malamulo onse amene ndikuuzani lero lino, kuti mukhale ndi moyo, ndi kucuruka, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova analumbirira makolo anu….
Akumbuke zokoma zazikuru Mulungu anawacitira 1 Muzisamalira kucita malamulo onse amene ndikuuzani lero lino, kuti mukhale ndi moyo, ndi kucuruka, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova analumbirira makolo anu….
1 Imvani Israyeli; mulikuoloka Yordano lero lino, kulowa ndi kulandira amitundu akuru ndi amphamvu akuposa inu, midzi yaikuru ndi ya malinga ofikira kuthambo, 2 anthu akuru ndi atalitali, ana a…
Za magome aciwiri a Malamulo 1 Masiku aja Yehova anati kwa ine, Dzisemere magome awiri amiyala onga oyamba aja, nukwere kuno kwa Ine m’phiriumu, nudzipangire likasa lamtengo. 2 Ndipo ndidzalembera…
1 Cifukwa cace muzikonda Yehova Mulungu wanu, ndi kusunga cilangizo cace, ndi malemba ace, ndi maweruzo ace, ndi malamulo ace, masiku onse. 2 Ndipo dziwani lero lino; pakuti sindinena ndi…
Malo Oyera akhale amodzi 1 Awa ndi malemba ndi maweruzo, muziwasamalirawa kuwacita m’dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani likhale lanu lanu, masiku onse akukhala ndi moyo inu pa…
Acenjere nao owanyenga kuwapembedzetsa mafano 1 Akauka pakati pa inu mneneri, kapena wakulota maloto, nakakupatsani cizindikilo kapena cozizwa; 2 ndipo cizindikilo kapena cozizwa adanenaci cifika, ndi kuti, Titsate milungu yina,…
Za nyama yodyedwa ndi yosadyedwa 1 Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu; musamadziceka, kapena kumeta tsitsi pakati pa maso cifukwa ca akufa. 2 Popeza ndinu mtundu wa anthu opatulikira…
Za caka ca cilekerero 1 Pakutha Pace pa zaka zisanu ndi ziwiri pakhale cilekerero. 2 Cilekereroco ndici: okongoletsa onse alekerere cokongoletsa mnansi wace; asacifunse kwa mnansi wace, kapena mbale wace;…
Madyerero a Paskha, a Masabata, ndi a Misasa 1 Samalirani mwezi wa Abibu, kuti muzicitira Yehova Mulungu wanu Paskha; popeza m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakuturutsani m’dziko la Aigupto…
1 Musamaphera Yehova Mulungu wanu nsembe ya ng’ombe, kapena nkhosa, yokhala naco cirema, kapena ciri conse coipa; pakuti cinyansira Yehova Mulungu wanu. 2 Akapeza pakati panu, m’mudzi wanu wina umene…