Numeri 34

Malire a dziko la Kanani 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati, 2 Uza ana Israyeli, nunene nao, Mutalowa a m’dziko la Kanani, ndilo dziko logwera inu, likhale colowa canu,…

Numeri 35

Midzi ya Alevi 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose m’zidikha za Moabu, pa Yordano, ku Yeriko, ndi kuti, 2 Uza ana a Israyeli, kuti apatseko Alevi colowa cao cao, midzi…

Numeri 36

Za kukwatibwa kwa ana akazi olandira colowa 1 Ndipo akuru a makolo a mabanja a ana a Gileadi, mwana wa Makiri, mwana wa Manase, wa mabanja a ana a Yosefe,…

Deuteronomo 1

Mose awafotokozera za ulendo wao m’cipululu 1 AWA ndi mau amene Mose ananena kwa Israyeli wonse, tsidya la Yordano m’cipululu, m’cidikha ca pandunji pa Sufu, pakati pa Parani, ndi Tofeli,…

Deuteronomo 2

1 Pamenepo tinabwerera, ndi kuyenda kumka kucipululu, kutsata njira ya Nyanja Yofiira, monga Yehova adanena ndi ine; ndipo tinapaza phiri la Seiri masiku ambiri. 2 Ndipo Yehova ananena ndi ine,…

Deuteronomo 3

1 Pamenepo tinatembenuka, ndi kubwera kumka njira ya ku Basana; ndipo Ogi mfumu ya Basana anaturuka kukomana nafe, kugwirana nafe nkhondo, iye ndi anthu ace onse, ku Edrei. 2 Ndipo…

Deuteronomo 4

Mose awadandaulira amvere Malamulo a Mulungu 1 Ndipo tsopano, Israyeli, dioloketu tamverani malemba ndi maweruzo, amene ndikuphunzitsani muwacite; kuti mukhale ndi moyo, ndi kulowa, ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu…

Deuteronomo 5

Mose abwereza kuwachulira Malamulo a Mulungu 1 Ndipo Mose anaitana Israyeli wonse, nanena nao, Tamverani, Israyeli, malemba ndi maweruzo ndinenawa m’makutu mwanu lero, kuti muwaphunzire, ndi kusamalira kuwacita. 2 Yehova…

Deuteronomo 6

Awapempha asunge Malamulo a Mulungu kuti adale 1 Ndipo awa ndi malamulo, malemba, ndi maweruzo, amene Yehova Mulungu wanu analamulira kukuphunzitsani, kuti muziwacita m’dziko limene muolokerako kulilandira; 2 kuti muope…

Deuteronomo 7

Awapangira za Akanani ndi zipembedzo zao 1 Pamene Yehova Mulungu wanu atakulowetsani m’dziko limene mumkako kulilandira likhale lanu lanu, ndipo atakataya amitundu ambiri pamaso panu, Ahiti, ndi Agirigazi, ndi Aamori,…