Numeri 14

Aisrayeli afuna kubwerera kumka ku Aigupto 1 Pamenepo khamu lonse linakweza mau ao, napfuula; ndipo anthuwo analira usikuwo. 2 Ndipo ana onse a Israyeli anadandaulira Mose ndi Aroni; ndi khamu…

Numeri 15

Malamulo a pa nsembezo 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose nati, 2 Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Mukakalowa m’dziko lokakhalamo inu, limene ndirikupatsa inu, 3 ndipo mukakonzera Yehova…

Numeri 16

Kora, Datani, ndi Abiramu aukira Mose 1 Koma Kora, mwana wa Izara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, anatenga Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu, ndi Oni mwana wa Peleti,…

Numeri 17

Ndodo ya Aroni iphuka 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati, 2 Nena ndi ana a Israyeli, nulandire kwa yense ndodo, banja liri onse la makolo ndodo imodzi, mafuko ao…

Numeri 18

Udindo wa ansembe ndi Alevi, ndi zolandira zao 1 Ndipo Yehova anati kwa Aroni, Iwe ndi ana ako amuna ndi banja la kholo lako pamodzi ndi iwe muzisenza mphulupulu ya…

Numeri 19

Za ng’ombe yamsoti yofiira ndi madzi oyeretsa nao 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati, 2 Ili ndi lemba la cilamulo Yehova adalamuliraci, ndi kuti, Nena ndi ana…

Numeri 20

Imfa ya Miriamu; madzi a Meriba 1 Ndipo ana a Israyeli, ndilo khamu lonse, analowa m’cipululu ca Zini mwezi woyamba; ndipo anthu anakhala m’Kadesi; kumeneko anafa Miriamu, naikidwakomweko. 2 Ndipo…

Numeri 21

Aisrayeli aononga Akanani 1 Pamene Mkanani, mfumu ya Aradi, wokhala kumwela, anamva kuti Israyeli anadzera njira ya azondi, anathira nkhondo pa Israyeli, nagwira ena akhale ansinga. 2 Ndipo Israyeli analonjeza…

Numeri 22

Za Balamu ndi Balaki 1 Ndipo ana a Israyeli anayenda ulendo, namanga mahema m’zigwa za Moabu, tsidya la Yordano ku Yeriko. 2 Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israyeli…

Numeri 23

1 Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Ndimangireni kuno maguwa a nsembe asanu ndi awiri, nimundikonzere kuno ng’ombe zisanu ndi ziwiri, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri. 2 Ndipo Balaki anacita…