Levitiko 21

Za kupatulika kwa ansembe 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Nena ndi ansembe, ana a Aroniwo, nuti nao, Asadzidetse mmodzi wa inu cifukwa ca wakufa mwa anthu a mtundu wace;…

Levitiko 22

Ansembe ayere pakudya zopatulika 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti, 2 Nena ndi Aroni ndi ana ace amuna, kuti azikhala padera ndi zinthu zopatulika za ana a Israyeli,…

Levitiko 23

Za nyengo zoikika za Yehova 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti, 2 Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Nyengo zoikika za Yehova zimene muzilalikira zikhale masonkhano opatulika,…

Levitiko 24

Za mafuta a nyalizo ndi mkate woonekera 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti, 2 Uza ana a Israyeli, kuti akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti aziwalitsa…

Levitiko 25

Za caka copumula dziko 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose m’phiri la Sinai, ndi kuti, 2 Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Mutakalowa m’dziko limene ndikupatsani, dzikoli lizisungira Yehova…

Levitiko 26

Malamulo, malonjezo, ndi macenjezo 1 Musamadzipangira mafano, kapena kudziutsira mafano osema, kapena coimiritsa, kapena kuika mwala wozokota m’dziko mwanu kuugwadira umene; popeza Ine ndine Yehova Mulungu wanu. 2 Musunge masabata…

Levitiko 27

Cowinda ndi ciombolo cace 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti, 2 Nena ndi ana a Israyeli, nuti nao, Pamene munthu acita cowinda ca padera, anthuwo azikhala a Yehova…

Numeri 1

Aisrayeli awerengedwa m’cipululu ca Sinai 1 NDIPO Yehova ananena ndi Mose m’cipululu ca Sinai, m’cihema cokomanako, tsiku loyamba la mwezi waciwiri, caka caciwiri ataturuka m’dziko la Aigupto, ndi kuti, 2…

Numeri 2

Malongosoledwe a cigono 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati, 2 Ana a Israyeli azimanga mahema ao yense ku mbendera yace, ya cizindikilo ca nyumba ya kholo lace;…

Numeri 3

Nchito ya Alevi 1 Mibadwo ya Aroni ndi Mose, tsiku lija Yehova ananena ndi Mose m’phiri la Sinai, ndi iyo. 2 Ndipo maina ao a ana amuna a Aroni ndi…