Cibvumbulutso 4
Masomphenya a mpando wacifumu wa Mulungu, akuru makumi awiri ndi anai, ndi zamoyo zinai 1 Zitatha izi ndinapenya, ndipo taonani, khomo lotseguka m’Mwamba, ndipo mau oyamba ndinawamva, ngati lipenga Iakulankhuia…
Masomphenya a mpando wacifumu wa Mulungu, akuru makumi awiri ndi anai, ndi zamoyo zinai 1 Zitatha izi ndinapenya, ndipo taonani, khomo lotseguka m’Mwamba, ndipo mau oyamba ndinawamva, ngati lipenga Iakulankhuia…
Buku losindikizika ndi zosindikiza zisanu ndi ziwiri. Mwanawankhosa yekha ayenera kulitsegula 1 Ndipo ndinaona m’dzanja lamanja la iye wakukhala pa mpando wacifumu buku lolembedwa m’kati ndi kunja kwace, losindikizika ndi…
Atsegula zosindikiza zisanu ndi cimodzi 1 Ndipo ndinaona pamene Mwanawankhosa anamasula cimodzi ca zizindikilo zisanu ndi ziwiri, ndipo ndinamva cimodzi mwa zamoyo zinai, nicinena, ngati mau a bingu, Idza. 2…
Aisrayeli okhulupirika alanditsidwa 1 Zitatha izi ndinao na angelo anai alinkuimirira pa ngondya zinai za dziko, akugwira mphepo zinai za dziko, kuti ingaombe mphepo padziko, kapena panyanja, kapena pa mtengo…
Atsegula cosindikiza cacisanu ndi ciwiri. Angelo asanu ndi awiri, ndi malipenga oyamba anai 1 Ndipo pamene anamasula cizindikilo cacisanu ndi ciwiri, munali cete m’Mwamba monga mwa nthawi ya ora latheka….
Lipenga lacisanu, tsoka loyamba 1 Ndipo mngelo wacisanu anaomba, ndipo ndinaona nyenyezi yocokera kumwamba idagwa padziko; ndipo anampatsa iye cifunguliro ca dzenje la phompho. 2 Ndipo anatsegula pa dzenje la…
Yohane adya buku locokera Kumwamba 1 Ndipo ndinaona mngelo wina wolimba alikutsika Kumwamba, wobvala mtambo; ndi utawaleza pamutu pace, ndi nkhope yace ngati dzuwa, ndi mapazi ace ngati mizati yamoto;…
Mboni ziwirt 1 Ndipoanandipatsa ine bango ngati ndodo, ndikuti, Tanyamuka, nuyese Kacisi wa Mulungu, ndi guwa la nsembe, ndi iwo akulambiramo. 2 Ndipo bwalo la kunja kwa Kacisi ulisiye padera,…
Za mkazi ndi cinjoka 1 Ndipo cizindikilo cacikuru cinaoneka m’mwamba; mkazi wobvekedwa dzuwa, ndi mwezi ku mapazi ace, ndi pamutu pace korona wa nyenyezi khumi ndi ziwiri; 2 ndipo anali…
Cirombo cakuturuka m’nyanja 1 Ndipo ndinaimirira pa mcenga wa nyanja. Ndipo ndinaona cirombo cirinkuturuka m’nyanja, cakukhala nazo nyanga khumi, ndi mitu isanu ow iwiri, ndi pa nyanga zace nduwira zacifumu…