Ahebri 8

Cipangano cakale ndi cofanizira ndi copita, Kristu ali Nkhoswe ya cipangano cosatha 1 Koma mutu wafzi tanenazi ndi uwu: Tiri naye Mkuruwansembe wotere, amene anakhala pa dzanja lamanja la mpando…

Ahebri 9

Nsembe za’cipangano cakale zidacitika kawiri kawiri, nsembe ya Yesu idacitika kamodzi kokha 1 Ndipo cingakhale cipangano coyambaci cinali nazo zoikika za kulambira, ndi malo opatulika a pa dziko lapansi. 2…

Ahebri 10

Pakuti cilamulo pokhala nao 1 mthunzi wa zokoma zirinkudza, osati cifaniziro ceni ceni ca zinthuzo, sicikhozatu, ndi nsembe zomwezi caka ndi caka, zimene azipereka kosalekeza, kuwayesera angwiro iwo akuyandikira. 2…

Ahebri 11

Mtima wa cikhulupiriro. Okhulupirira a m’Cipangano cakale 1 Koma cikhulupiriro ndico cikhazikitso ca zinthu zoyembekezeka, ciyesero ca zinthu zosapenyeka. 2 Pakuti momwemo akulu anacitidwa umboru. 3 Ndi cikhulupiriro tizindikira kuti…

Ahebri 12

Tipirire angakhale masautso acuruka, monga anatero Kristu 1 Cifukwa cace ifenso, popeza tizingidwa nao mtambo waukuru wotere wa mboni, titaye colemetsa ciri conse, ndi cimoli Iimangotizinga, ndipo tithamange mwacipiriro makaniwo…

Ahebri 13

1 Cikondi ca pa abale cikhalebe. 2 Musaiwale kucereza alendo; pakuti mwa ici ena anacereza angelo osacidziwa. 3 Kumbukilani am’nsinga, monga am’nsinga anzao; ocitidwa zoipa, monga ngati inunso adatero nanu…

Yakobo 1

1 YAKOBO, kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Kristu, kwa mafuko khumi ndi awiri a m’cibalaliko: ndikulankhulani. Za mayesero 2 Muciyese cimwemwe cokha, abale anga, m’mene mukugwa m’mayesero a…

Yakobo 2

Asacite tsankhu pakati pa anthu 1 Abate anga, musakhale naco cikhulupiriro ca Ambuye wathu Yesu Kristu, Ambuye wa ulemerero, ndi kusamala maonekedwe. 2 Pakuti akalowa m’sunagoge mwanu munthu wobvala mphete…

Yakobo 3

Aziceniera ndi pakamwa pao 1 Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa. 2 Pakuti timakhumudwa tonse pa zinthu zambiri. Munthu akapanda kukhumudwa pa mau, iye ndiye munthu wangwiro,…

Yakobo 4

Adziletse polakalaka zoipa 1 Zicokera kuti nkhondo, zicokera kuti zolimbana mwa inu? Kodi sizicokera ku zikhumbitso zanu zocita nkhondo m’ziwalo zanu? 2 Mulakalaka, ndipo zikusowani; mukupha, nimucita kaduka, ndipo simukhoza…