1 Timoteo 2
Pempherero la kwa anthu onset 1 Ndidandaulira tsono, poyambayamba, kuti acitike mapembedzo, mapemphero, mapembedzero, mayamiko, cifukwa ca anthu onse; 2 cifukwa ca mafumu ndi onse akucita ulamuliro kuti m’moyo mwathu…
Pempherero la kwa anthu onset 1 Ndidandaulira tsono, poyambayamba, kuti acitike mapembedzo, mapemphero, mapembedzero, mayamiko, cifukwa ca anthu onse; 2 cifukwa ca mafumu ndi onse akucita ulamuliro kuti m’moyo mwathu…
Zoyenera oyang’anira ndi atumiki 1 Mauwa ali okhulupirika, ngati munthu akhumba udindo wa woyang’anira, aifuna nchito yabwino. 2 Ndipo kuyenera woyang’anira akhale wopanda cirema, mwamuna wa mkazi mmodzi, wodzisunga, wodziletsa,…
Cipanduko ca m’masiku otsiriza 1 Koma Mzimu anena monenetsa, kuti m’masiku otsiriza ena adzataya cikhulupiriro, ndi kusamala mizimu yosoceretsa ndi maphunziro a ziwanda, 2 m’maonekedwe onyenga a iwo onena mabodza,…
Za okalamba ndi amasiye 1 Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale; 2 akazi akulu ngati amai; akazi ang’ono ngati alongo, m’kuyera mtima konse. 3 Citira ulemu amasiye…
Zoyenera akapolo 1 Onse amene ali akapolo a m’goli, ayesere ambuye a iwo okha oyenera ulemu wonse, kuti dzina la Mulungu ndi ciphunzitso zisacitidwe mwano. 2 Ndipo iwo akukhala nao…
1 PAULO a mtumwi wa Kristu Yesu mwa cifuniro ca Mulungu, monga mwa lonjezano la moyo wa m’Kristu Yesu, 2 kwa Timoteo, mwana wanga wokondedwa: Cisomo, cifundo, mtendere za kwa…
1 Ndipo iwe, mwana wanga, limbika m’cisomo ca m’Kristu Yesu. 2 Ndipo zimene wazimva kwa ine mwa mboni zambiri, zomwezi uikize kwa anthu okhulupirika, amene adzadziwa kuphunzitsa enanso. 3 Umve…
Zoipa zoopsa masiku otsiriza 1 Koma zindikira ici, kuti masiku otsiriza zidzafika nthawi zowawitsa. 2 Pakuti anthu adzakhala odzikonda okha, okonda ndarama, odzitamandira, odzikuza, amwano, osamvera akuwabala, osayamika, 3 osayera…
1 Ndikucitira umboni pamaso pa Mulungu ndi Kristu Yesu, amene adzaweruza amoyo ndi akufa, ndi pa maonekedwe ace ndi ufumu wace; 2 lalikira mau; cita nao pa nthawi yace, popanda…
1 PAULO, kapolo wa Mulungu ndi mtumwi wa Yesu Kristu monga mwa cikhulupiriro ca osa nkhika a Mulungu, ndi cizindikiritso ca coonadi ciri monga mwa cipembedzo, 2 m’ciyembekezo ca moyo…