Akolose 4

1 Ambuye inu, citirani akapolo anu colungama ndi colingana; podziwa kuti inunso muli naye Mbuye m’Mwamba. Awacenjeza za kupemphera ndi za kukhala nayo nzeru 2 Citani khama m’kupemphera, nimudikire momwemo…

1 Atesalonika 1

1 PAULO, ndi Silvano, ndi Timoteo, kwa Mpingo wa Atesalonika mwa Mulungu Atate ndi Ambuye Yesu Kristu: Cisomo kwa inu ndi mtendere. Zipatso za Uthenga Wabwino ku Tesalonika 2 Tiyamika…

1 Atesalonika 2

Za utumiki wace wa kwa Atesalonika 1 Pakuti, abale, mudziwa nokha malowedwe athu a kwa inu, kuti sanakhala opanda pace; 2 koma tingakhale tidamva zowawa kale, ndipo anaticitira cipongwe, monga…

1 Atesalonika 3

1 Cifukwa cace, posakhoza kulekereranso, tidabvomereza mtima atisiye tokhaku Atene; 2 ndipo tinatuma Timoteo, mbale wathuyo ndi mtumiki wa Mulungu m’Uthenga Wabwino wa Kristu, kuti akhazikitse inu; ndi kutonthoza inu…

1 Atesalonika 4

Atsate kuyera-mtima, cikondano, ndi khama 1 Cotsalira tsono, abale, tikupemphani ndi kukudandaulirani mwa Ambuye Yesu, kuti, monga munalandira kwa ife mayendedwe okoma, muyenera kuyendanso ndi kukondweretsa Mulungu, monganso mumayenda, eurukani…

1 Atesalonika 5

1 Koma za nthawizo ndi nyengozo, abale, sikufunika kuti tidzakulemberani, 2 Pakuti inu nokha mudziwa bwino kuti tsiku la Ambuye lidzadza monga mbala usiku, 3 Pamene angonena, Mtendere ndi mosatekeseka,…

2 Atesalonika 1

1 PAULO, ndi Silvano, ndi Timoteo, kwa Mpingo wa Atesalonika mwa Mulungu Atate wathu ndi Ambuye Yesu Kristu: 2 Cisomo kwa inu ndi mtendere wa kwa Mulungu Atate ndi Ambuye…

2 Atesalonika 2

Asanabwere Kristu adzaoneka wokana Kristu 1 Ndipo tikupemphani, abale, cifukwa ca kudza kwace kwa Ambuye wathu Yesu Kristu, ndi kusonkhana pamodzi kwathu kwa iye; 2 kuti musamagwedezeka mtima msanga ndi…

2 Atesalonika 3

Zowacenieza ndi malankhulano 1 Cotsalira, abale, mutipempherere, kuti mau a Ambuye athamange, nalemekezedwe, monganso kwanu; 2 ndi kuti tilanditsidwe m’manja a anthu osayenerandi oipa; pakuti si onse ali naco cikhulupiriro….

1 Timoteo 1

Paulo alangiza Timoteo 1 PAULO, mtumwi wa Kristu Yesu monga mwa cilamuliro ca Mulungu Mpulumutsi wathu, ndi ca Kristu Yesu, ciyembekezo cathu: 2 kwa Timoteo mwana wanga weniweni m’cikhulupiriro: Cisomo,…