2 Akorinto 3
1 Kodi tirikuyambanso kudzibvomereza tokha? kapena kodi tisowa, monga ena, akalata otibvomerezetsa kwa inu, kapena ocokera kwa inu? 2 Inu ndinu kalata wathu, wolembedwa mu mitima yathu, wodziwika ndi wowerengedwa…
1 Kodi tirikuyambanso kudzibvomereza tokha? kapena kodi tisowa, monga ena, akalata otibvomerezetsa kwa inu, kapena ocokera kwa inu? 2 Inu ndinu kalata wathu, wolembedwa mu mitima yathu, wodziwika ndi wowerengedwa…
Paulo alalikira Yesu yekha yekha 1 Cifukwa cace popeza tiri nao utumiki umene, monga talandira cifundo, sitifoka; 2 koma takaniza zobisfka za manyazi, osayendayenda mocenjerera, kapena kucita nao mau a…
1 Pakuti tidziwa kuti ngati nyumba ya pansi pano ya msasa wathu ipasuka, tiri naco cimango ca kwa Mulungu, ndiyo nyumba yosamangidwa ndi manja, yosatha, m’Mwamba. 2 Pakutinso m’menemo tibuula,…
Kudzikana kwa Paulo m’utumiki wace 1 Ndipo a ocita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire cisomo ca Mulungu kwacabe inu, 2 (pakuti anena, M’nyengo yolandiridwa ndinamva iwe, Ndipo m’tsiku la cipulumutso…
Paulo akondwerapa kudza kwa Tito, ndi pa zipatso za kalata wace woyamba 1 Pokhala nao tsono malonjezano amenewa, okondedwa, tidzikonzere tokha kuleka codetsa conse ca thupi ndi ca mzimu, ndi…
Cipereko ca kwa Akristu aumphawi a ku Yerusalemu 1 Ndipo tikudziwitsani, abale, cisomo ca Mulungu copatsika mwa Mipingo ya ku Makedoniya, 2 kuti m’citsimikizo cacikuru ca cisautso, kucurukitsa kwa cimwemwe…
1 Pakutitu za utumiki wa kwa oyera mtima sikufunika kwa ine kulembera inu; 2 pakuti ndidziwa cibvomerezo canu cimene ndidzitamandira naco cifukwa ca inu ndi Amakedoniya, kuti Akaya anakonzekeratu citapita…
Ulamuliro wa Paulo mtumwi 1 Koma ine ndekha Paulo, ndidandaulira inu mwa kufatsa ndi ulere wa Kristu, ine amene pamaso panu ndikhala wodzicepetsa pakati pa inu, koma pokhala kwina ine…
Za atumwi onyenga 1 Mwenzi mutandilola pang’ono ndi copusaco! Komanso mundilole. 2 Pakuti ndicita nsanje pa inu ndi nsanje ya Mulungu; pakuti ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna mmodzi, kuti ndikalangize inu ngati…
Masomphenya a Paulo ndi munga m’thupi lace 1 Ndiyenera kudzitamandira, kungakhale sikupindulika; koma ndidzadza ku masomphenya ndi mabvumbulutso a Ambuye. 2 Ndidziwa munthu wa mwa Kristu, zitapita zaka khumi ndi…