1 Akorinto 9
Ululu ndi ulamuliro wa mtumwiyo 1 Kodi sindine mfulu? Kodi slndine mtumwi? Kodi sindinaona Yesu Ambuye wathu? Kodi simuli inu nchito yanga mwa Ambuye? 2 Ngati sindiri mtumwi kwa ena,…
Ululu ndi ulamuliro wa mtumwiyo 1 Kodi sindine mfulu? Kodi slndine mtumwi? Kodi sindinaona Yesu Ambuye wathu? Kodi simuli inu nchito yanga mwa Ambuye? 2 Ngati sindiri mtumwi kwa ena,…
Tisayese dala Mulungu monga Israyeli 1 Pakuti sindifuna, kuti mukhale osadziwa, abale, kuti makolo athu onse anali pansi pa mtambo, naoloka nyanja onse; 2 nabatizidwa onse kwa Mose, mumtambo, ndi…
1 Khalani onditsanza ine, monga inenso oditsanza Kristu. Za akazi m’Eklesia wa Ambuye 2 Ndipo ndikutamandani kuti m’zinthu zonse mukumbukila ine, ndi kuti musunga miyambo monga ndinapereka kwa inu. 3…
Mphatso ta Mzimu zisiyana 1 Koma za mphatso zauzimu, abale, sindifuna kuti mukhale osadziwa. 2 Mudziwa kuti pamene munali amitundu, munatengedwa kunka kwa mafano aja osalankhula, monga munatsogozedwa. 3 Cifukwa…
Kuposa kwa Cikondi 1 Ndingakhale ndilankhula malilime a anthu, ndi a angelo, koma ndiribe cikondi, ndikhala mkuwa woomba, kapena nguli yolira. 2 Ndipo ndingakhale ndikhoza kunenera, ndipo ndingadziwe zinsinsi zonse,…
Mpnatso ya kunenera tposa ya malilime 1 Tsatani cikondi; koma funitsitsani mphatsozauzimu, koma koposa kuti mukanenere. 2 Pakuti iye wakulankhula lilime salankhula ndi anthu, koma ndi Mulungu; pakuti palibemunthu akumva;…
Za kuuka kwa akufa 1 Ndipo ndikudziwitsani, abale, Uthenga Wabwino umene ndinakulalikirani inu, umenenso munalandira, umenenso muimamo, 2 umenenso mupulumutsidwa nao ngati muugwiritsa monga momwe ndinalalikira kwa inu; ngati simunakhulupira…
Zopereka za kwa Akristu a ku Yerusalemu 1 Koma za copereka ca kwa oyera mtima, mongandinalangiza Mipingo ya ku Galatiya, motero citani inunso. 2 Tsiku loyamba la sabata yense wa…
1 PAULO, mtumwi wa Kristu Yesu, mwa cifuniro ca Mulungu, ndi Timoteo mbaleyo, kwa Mpingo wa Mulungu umene uli ku Korinto, pamodzi ndi oyera mtima onse amene ali m’Akaya lonse:…
1 Koma ndinatsimikiza mtima mwa ine ndekha, ndisadzenso kwa inu ndi cisoni. 2 Pakuti ngati ine ndimvetsa inu cisoni, ndaninso amene adzandikondweretsa ine, kama iye amene ndammvetsa cisoni? 3 Ndipo…