Zekariya 11

Kulangidwa kwa osalapa 1 Tsegula pa makomo ako Lebano, kuti moto uthe mikungudza yako. 2 Cema, mtengo wamlombwa, pakuti mkungudza wagwa, popeza mitengo yokoma yaipitsidwa; cemani athundu a ku Basani,…

Zekariya 12

Ukulu wa Israyeli m’tsogolo 1 Katundu wa mau a Yehova wakunena Israyeli. Atero Yehova, wakuyala miyamba, ndi kuika maziko a dziko lapansi, ndi kulenga mzimu wa munthu m’kati mwace; 2…

Zekariya 13

Kuyeretsedwa kwa Yerusalemu 1 Tsiku lomwelo padzatsegukira nyumba ya Davide ndi okhala m’Yerusalemu kasupe wa kwa ucimo ndi cidetso. 2 Ndipo kudzacitika tsiku lomwelo, ati Yehova wa makamu, ndidzaononga maina…

Zekariya 14

Yehova adzathandiza a ku Yerusalemu polimbana ndi amitundu 1 Taonani likudza tsiku la Yehova, limene zofunkha zako zidzagawanika pakati pako. 2 Pakuti ndidzasonkhanitsa amitundu onse alimbane ndi Yerusalemu; ndipo mudziwo…