Zefaniya 1

Mau oopsa akucenjeza Yerusalemu ndi Yuda 1 MAU a Yehova amene anadza kwa Zefaniya mwana wa Kusi, mwana wa Gedaliya, mwana wa Amariya, mwana wa Hezekiya, masiku a Yosiya, mwana…

Zefaniya 2

Mau akucenjeza amitundu ena 1 Dzisanthuleni, inde santhulani; inu mtundu wosakhumba kanthu; 2 lamulo lisanabale, tsiku lisanapitirire ngati mungu, usanakugwereni mkwiyo waukali wa Yehova, lisanakugwereni tsiku la mkwiyo wa Yehova….

Zefaniya 3

Mau akudzudzula Yerusalemu. Malonjezo a kwa okhulupirika otsala 1 Tsoka uyo wopanduka, ndi wodetsedwa, ndiye mudzi wozunza! 2 Sanamvera mau, sanalola kulangizidwa; sanakhulupirira Yehova, sanayandikira kwa Mulungu wace. 3 Akalonga…