Yuda 1

1 YUDA, kapolo wa Yesu Kristu, ndi mbale wa Yakobo, kwa iwo oitanidwa, okondedwa mwa Mulungu Atate, ndi osungidwa ndi Yesu Kristu: 2 Cifundo ndi mtendere ndi cikondi zikucurukireni. Atsutsa…