Yobu 11

Zofari adzudzula Yobu pa kudzilungamitsa kwace, namcenjeza alape 1 Pamenepo anayankha Zofari wa ku Naama, nati, 2 Kodi mau ocurukawa sayenera kuwayankha? Ndi munthu wa milomo ayenera kuyesedwa wolungama? 3…

Yobu 12

Yobu abvomerezanso ukulu wa Mulungu, koma mau a abwenziwo ndi opanda pace; nanena za moyo wa munthu ukutha msanga 1 Pamenepo Yobu anayankha, nati, 2 Zoonadi inu ndinu anthu, Ndi…

Yobu 13

1 Taonani; diso langa laciona conseci; M’khutu mwanga ndacimva ndi kucizindikira. 2 Cimene mucidziwa inu, inenso ndicidziwa; Sindikuceperani. 3 Koma ine ndidzanena ndi Wamphamvuyonse, Ndipo ndifuna kudzikanira kwa Mulungu. 4…

Yobu 14

1 Munthu wobadwa ndi mkazi Ngwa masiku owerengeka, nakhuta mabvuto, 2 Aturuka ngati duwa, nafota; Athawa ngati mthunzi, osakhalitsa. 3 Ndipo kodi mumtsegulira maso anu wotereyo, Ndi kunditenga kunena nane…

Yobu 15

Elifazi atsutsa Yobu pa kudzikuza kwace. Akuti, akuru omwe atsimikiza kuti ocimwa sakhala bwino 1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha, nati, 2 Kodi mwini nzeru ayankhe ndi kudziwa kouluzika,…

Yobu 16

Yobu atonza mabwenziwo kuti mau ao samthandiza, akana kuti sanacimwa, nadziponya kwa Mulungu. Ciyembekezo cace ndi imfa 1 Pamenepo Yobu anayankha, nati, 2 Ndamva zambiri zotere; Inu nonse ndinu otonthoza…

Yobu 17

1 Mzimu wanga watha, masiku anga afafanizika, Kumanda kwandikonzekeratu. 2 Zoonadi, ali nane ondiseka; Ndi diso langa liri cipenyere m’kundiwindula kwao. 3 Mupatse cigwiriro tsono, mundikhalire cikole Inu nokha kwanu;…

Yobu 18

Bilidadi atsutsa Yobu pa kudzikuza kwace, nanena za tsoka la oipa 1 Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha, nati, 2 Musaka mau kufikira liti? Zindikirani, ndi pamenepo tidzanena. 3 Tiyesedwa…

Yobu 19

Yobu achulira mabwenzi ace matsoka ace, napempha amcitire cifundo, Adzitonthoza ndi Mpulumutsi wace 1 Koma Yobu anayankha, nati, 2 Mudzasautsa moyo wanga kufikira liti, Ndi kundityolatyola nao mau? 3 Kakumi…

Yobu 20

Zofari afotokozera masautso amene Mulungu atumizira oipa 1 Pamenepo anayankha Zofari Mnaama, nati, 2 M’mwemo zolingirira zanga zindiyankha, Cifukwa cace ndifulumidwa m’kati mwanga. 3 Ndamva kudzudzula kwakundicititsa manyazi, Ndi mzimu…