Yesaya 31
Toka otama cithandizo ca Aigupto 1 Tsoka kwa iwo amene atsikira kunka ku Aigupto kukathandizidwa, natama akavalo; nakhulupirira magareta, pakuti ali ambiri, ndi okwera pa akavalo, pakuti ali a mphamvu…
Toka otama cithandizo ca Aigupto 1 Tsoka kwa iwo amene atsikira kunka ku Aigupto kukathandizidwa, natama akavalo; nakhulupirira magareta, pakuti ali ambiri, ndi okwera pa akavalo, pakuti ali a mphamvu…
Ufumu wa mfumu yolungama 1 Taonani mfumu idzalamulira m’cilungamo, ndi akalonga adzalamulira m’ciweruzo. 2 Ndipo munthu adzakhala monga pobisalira mphepo, ndi pousira cimphepo; monga mitsinje yamadzi m’malo ouma, monga mthunzi…
Adani a anthu a Mulungu adzapasuka; Yerusalemu adzabwezedwa ulemu 1 Tsoka kwa iwe amene usakaza, cinkana sunasakazidwa; nupangira ciwembu, cinkana sanakupangira iwe ciwembu! Utatha kusakaza, iwe udzasakazidwa; ndipo utatha kupangira…
Yehova aipidwa ndi amitundu 1 Idzani pafupi, amitundu inu, kuti mumve; mverani anthu inu, dziko limve, ndi za mommo; dziko ndi zinthu zonse zoturukamo. 2 Pakuti Yehova akwiyira amitundu onse,…
Cikondwerero ca Ziyoni m’tsogolomo 1 Cipululu ndi malo ouma adzakondwa; ndipo dziko loti se lidzasangalala ndi kuphuka ngati duwa. 2 Lidzaphuka mocuruka ndi kusangalala, ngakhale kukondwa ndi kuyimba; lidzapatsidwa ulemerero…
Nkhondo ya Sanakeribu idzera Yerusalemu 1 Koma panali caka cakhumi ndi cinai ca mfumu Hezekiya, Sanakeribu, mfumu ya Asuri anadza, nathira nkhondo pa midzi ya malinga yonse ya Yuda, nailanda….
Mwa mantha Hezekiya aitana mnenert Yesaya 1 Ndipo panali pamene mfumu Hezekiya anamva, anang’amba zobvala zace, nabvala ciguduli, nalowa m’nyumba ya Yehova. 2 Ndipo anatumiza Eliakimu, wapanyumba, ndi Sebina, mlembi,…
Kudwala kwa Hezekiya ndi kuciritsidwa kwace 1 Masiku amenewo Hezekiya anadwala, nafuna kufa. Ndipo Yesaya mneneri, mwana wa Amozi, anadza kwa iye, nati kwa iye, Atero Yehova, Konza nyumba yako,…
Hezekiya aonetsa amithenga a ku Babulo cuma cace, Yesaya namdzudzula 1 Nthawi imeneyo Merodakibaladani, mwana wa Baladani, mfumu ya ku Babulo, anatumiza akalata ndi mphatso kwa Hezekiya; pakuti anamva kuti…
Lonjezo la cipulumutso ca Israyeli 1 Mutonthoze, mutonthoze mtima wa anthu anga, ati Mulungu wanu. 2 Munene inu zotonthoza mtima kwa Yerusalemu, nimupfuulire kwa iye, kuti nkhondo yace yatha, kuti…