Yeremiya 41

Gedaliya ndi ena aphedwa ndi Ismayeli 1 Ndipo panali mwezi wacisanu ndi ciwiri, Ismayeli mwana wa Netaniya, mwana wa Elisama, wa mbeu ya mfumu, ndi kapitao wamkuru wa mfumu, ndi…

Yeremiya 42

Yeremiya acenjeza anthu asapite ku Aigupto 1 Ndipo akazembe onse a nkhondo, ndi Yohanani mwana wace wa Kareya, ndi Jezaniya mwana wace wa Hosiya, ndi anthu onse kuyambira wamng’ono, kufikira…

Yeremiya 43

Amtenga Yeremiya napita naye ku Aigupto 1 Ndipo panali pamene Yeremiya anatha kunena kwa anthu onse mau onse a Yehova Mulungu wao, amene anamtuma iye nao Yehova Mulungu wao, mau…

Yeremiya 44

Acenjeza mowaopsa Ayuda amene adathawira ku Aigupto 1 Mau amene anadza kwa Yeremiya onena za Ayuda onse amene anakhala m’dziko la Aigupto, okhala pa Migidoli, ndi pa Tapanesi, ndi pa…

Yeremiya 45

Mau a Mulungu kwa Baruki 1 Mau amene ananena Yeremiya mneneri kwa Baruki mwana wace wa Neriya, pamene analemba mau awa m’buku ponena Yeremiya, caka cacinai ca Yehoyakimu mwana wace…

Yeremiya 46

Aneneratu kuti mfumu ya ku Babulo idzagonjetsa Aaigupto 1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu. 2 Za Aigupto: kunena za nkhondo ya Farao-neko mfumu ya…

Yeremiya 47

Aneneratu za citsutso ca Afilisti 1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri onena za Afilisti, Farao asanakanthe Gaza. 2 Yehova atero: Taonani, madzi adzakwera kuturuka kumpoto, nadzakhala mtsinje…

Yeremiya 48

Citsutso ca Moabu 1 Za Moabu Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli: Tsoka Nebo! pakuti wapasuka; Kiriyataimu wacitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lacitidwa manyazi lapasudwa. 2 Palibenso kutamanda…

Yeremiya 49

Citsutso ca Aamoni 1 Za ana a Amoni. Yehova atero: Kodi Israyeli alibe ana amuna? alibe wolowa dzina? M’mwemo mfumu yao yalowa pa Gadi cifukwa canji, ndi anthu ace akhala…

Yeremiya 50

Citsutso ca Babulo 1 Mau amene ananena Yehova za Babulo, za dziko la Akasidi, mwa Yeremiya mneneri. 2 Lalikirani mwa amitundu, falikitsani, kwezani mbendera; falikitsani, musabise; munene, Babulo wagwidwa, Beli…