Yakobo 1

1 YAKOBO, kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Kristu, kwa mafuko khumi ndi awiri a m’cibalaliko: ndikulankhulani. Za mayesero 2 Muciyese cimwemwe cokha, abale anga, m’mene mukugwa m’mayesero a…

Yakobo 2

Asacite tsankhu pakati pa anthu 1 Abate anga, musakhale naco cikhulupiriro ca Ambuye wathu Yesu Kristu, Ambuye wa ulemerero, ndi kusamala maonekedwe. 2 Pakuti akalowa m’sunagoge mwanu munthu wobvala mphete…

Yakobo 3

Aziceniera ndi pakamwa pao 1 Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa. 2 Pakuti timakhumudwa tonse pa zinthu zambiri. Munthu akapanda kukhumudwa pa mau, iye ndiye munthu wangwiro,…

Yakobo 4

Adziletse polakalaka zoipa 1 Zicokera kuti nkhondo, zicokera kuti zolimbana mwa inu? Kodi sizicokera ku zikhumbitso zanu zocita nkhondo m’ziwalo zanu? 2 Mulakalaka, ndipo zikusowani; mukupha, nimucita kaduka, ndipo simukhoza…

Yakobo 5

Acuma ouma mtima atsutsidwa 1 Nanga tsono acuma inu, lirani ndi kucema cifukwa ca masautso anu akudza pa inu, 2 Cuma canu caola ndi zobvala zanu zajiwa ndi njenjete. 3…