Rute 1

Naomi ndi apongozi ace awiri 1 NDIPO masiku akuweruza oweruzawo munali njala m’dziko. Ndipo munthu wa ku Betelehemu-Yuda anamuka nakagonera m’dziko la Moabu, iyeyu, ndi mkazi wace, ndi ana ace…

Rute 2

Rute akunkha m’munda wa Boazi 1 Ndipo Naomi anali nave mbale wa mwamuna wace, ndiye munthu mwini cuma cambiri wa banja la Elimeleki; dzina lace ndiye Boazi. 2 Nati Rute…

Rute 3

Boazi anena za kumuombolera Rute colowa 1 Pamenepo Naomi mpongozi wace ananena naye, Mwana wanga, kodi ndisakufunire popumulako, kuti ukhale bwino? 2 Nanga Boazi wodziwana nafe, amene unakhala nao adzakazi…

Rute 4

Boazi akwatira Rute nabadwa Obedi 1 Ndipo Boazi anakwera kumka kucipata, nakhala pansi pomwepo; ndipo taona, woombolera winayo adanena Boazi analinkupita; nati iye, Iwe uje, pambuka, khala pansi apa; napambuka…