Numeri 21
Aisrayeli aononga Akanani 1 Pamene Mkanani, mfumu ya Aradi, wokhala kumwela, anamva kuti Israyeli anadzera njira ya azondi, anathira nkhondo pa Israyeli, nagwira ena akhale ansinga. 2 Ndipo Israyeli analonjeza…
Aisrayeli aononga Akanani 1 Pamene Mkanani, mfumu ya Aradi, wokhala kumwela, anamva kuti Israyeli anadzera njira ya azondi, anathira nkhondo pa Israyeli, nagwira ena akhale ansinga. 2 Ndipo Israyeli analonjeza…
Za Balamu ndi Balaki 1 Ndipo ana a Israyeli anayenda ulendo, namanga mahema m’zigwa za Moabu, tsidya la Yordano ku Yeriko. 2 Ndipo Balaki mwana wa Zipori anaona zonse Israyeli…
1 Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Ndimangireni kuno maguwa a nsembe asanu ndi awiri, nimundikonzere kuno ng’ombe zisanu ndi ziwiri, ndi nkhosa zamphongo zisanu ndi ziwiri. 2 Ndipo Balaki anacita…
1 Pamene Balamu anaona kuti kudakomera pamaso pa Yehova kudalitsa Israyeli, sanamuka, monga nthawi zija zina, ku nyanga zolodzera, koma anayang’ana nkhope yace kucipululu. 2 Ndipo Balamu anakweza maso ace,…
Aisrayeli acita cigololo napembedza mafano ku Sitimu 1 Ndipo Israyeli anakhala m’Sitimu, ndipo anthu anayamba kucita cigololo ndi ana akazi a Moabu; 2 popeza anaitana anthuwo adze ku nsembe za…
Awerenzedwa Aisrayeli 1 Ndipo kunali, utatha mliriwo, Yehova ananena ndi Mose ndi Eleazara mwana wa Aroni wansembe, nati, 2 Werenga khamu lonse la ana a Israyeli, kuyambira a zaka makumi…
Ana akazi a Tselofekadi 1 Pamenepo anayandikiza ana akazi a Tselofekadi mwana wa Heferi, ndiye mwana wa Gileadi, ndiye mwana wa Makiri, ndiye mwana wamwamuna wa Manase, wa mabanja a…
Nsembe yopsereza yosalekeza 1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati, 2 Uza ana a Israyeli, nuti nao, Muzisamalira kubwera naco kwa Ine copereka canga, cakudya canga ca nsembe zanga zamoto,…
1 Ndipo mwezi wacisanu ndi ciwiri, tsiku loyamba la mweziwo, muzikhala nako kusonkhana kopatulika; musamacita nchito ya masiku ena; likukhalireni inu tsiku lakuliza malipenga. 2 Pamenepo muzipereka nsembeyopsereza ya pfungo…
Za cowinda cocita akazi 1 Ndipo Mose ananena ndi akuru a mapfuko a ana a Israyeli, nati, Cinthu anacilamulira Yehova ndi ici: 2 Munthu akacitira Yehovacowinda, kapena akalumbira lumbiro ndi…