Nehemiya 11

Ena akhala m’Yerusalemu, ena m’midzi yina 1 Ndipo akuru anthu anakhala m’Yerusalemu; anthu otsala omwe anacita maere, kuti libwere limodzi la magawo khumi likhale m’Yerusalemu, mudzi wopatulika, ndi asanu ndi…

Nehemiya 12

Maina a ansembe ndi Alevi ofika ku Yerusalemu pamodzi ndi Zerubabele 1 Ndipo ansembe ndi Alevi amene anakwera ndi Zerubabele mwana wa Sealtiyeli, ndi Yesuwa, ndi awa: Seraya, Yeremiya, Ezara,…

Nehemiya 13

Tobiya acotsedwa ku Kacisi 1 Tsiku lomwelo anawerenga m’buku la Mose m’makutu a anthu, napeza m’menemo kuti Aamoni ndi Amoabu asalowe mu msonkhano wa Mulungu ku nthawi yonse; 2 popeza…