Nahumu 1
Cilungamo ndi cifundo ca Mulungu. Adzaononga adani ndi kulanditsa anthu ace 1 KATUNDU wa Nineve. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi. 2 Yehova ndiye Mulungu wansanje, nabwezera cilango;…
Cilungamo ndi cifundo ca Mulungu. Adzaononga adani ndi kulanditsa anthu ace 1 KATUNDU wa Nineve. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi. 2 Yehova ndiye Mulungu wansanje, nabwezera cilango;…
Nineve amangidwa misasa nalandidwa 1 Wophwanyayo wakwera pamaso pako; sunga linga, yang’anira panjira, limbitsa m’cuuno mwako, limbikitsatu mphamvu yako. 2 Pakuti Yehova abwezeranso ukulu wace wa Yakobo ngati ukulu wace…
Zoipa za Nineve ndi kupasuka kwace 1 Tsoka mudzi wa mwazi! udzala nao mabodza ndi zacifwamba; zacifwamba sizidukiza. 2 Kumveka kwa cikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magareta;…