Miyambi 11
1 Muyeso wonyenga unyansa Yehova; Koma mulingo wamphumphu umsekeretsa. 2 Pakudza kudzikuza padzanso manyazi; Koma nzeru iri ndi odzicepetsa, 3 Kuongoka mtima kwa olungama kuwatsogolera; Koma kukhota kwa aciwembu kudzawaononga….
1 Muyeso wonyenga unyansa Yehova; Koma mulingo wamphumphu umsekeretsa. 2 Pakudza kudzikuza padzanso manyazi; Koma nzeru iri ndi odzicepetsa, 3 Kuongoka mtima kwa olungama kuwatsogolera; Koma kukhota kwa aciwembu kudzawaononga….
1 Wokonda mwambo akonda kudziwa; Koma wakuda cidzudzulo apulukira. 2 Yehova akomera mtima munthu wabwino; Koma munthu wa ziwembu amtsutsa, 3 Munthu sadzakhazikika ndi udio, Muzu wa olungama sudzasunthidwa. 4…
1 Mwana wanzeru amamvera mwambo wa atate; Koma wonyoza samvera cidzudzulo. 2 Munthu adzadya zabwino ndi zipatso za m’kamwa mwace; Koma moyo wa aciwembu udzadya ciwawa. 3 Wogwira pakamwa pace…
1 Mkazi yense wanzeru amanga banja lace; Koma wopusa alipasula ndi manja ace. 2 Woyenda moongoka mtima aopa Yehova; Koma wokhota m’njira yace amnyoza, 3 M’kamwa mwa citsiru muli ntyole…
1 Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; Koma mau owawitsa aputa msunamo. 2 Lilime la anzeru linena bwino zomwe adziwa; Koma m’kamwa mwa opusa mutsanulira utsiru. 3 Maso a Yehova ali ponseponse,…
1 Malongosoledwe a mtima nga munthu; Koma mayankhidwe a lilime acokera kwa Yehova. 2 Njira zonse za munthu ziyera pamaso pace; Koma Yehova ayesa mizimu. 3 Pereka zocita zako kwa…
1 Nyenyeswa youma, pokhala mtendere, Iposa nyumba yodzala nyama yansembe, pali makangano. 2 Kapolo wocitamwanzeru Adzalamulira mwana wocititsa manyazi, Nadzagawana nao abale colowa. 3 Siliva ali ndi mbiya yosungunulira, golidi…
1 Wopanduka afunafuna niro cace, Nakangana ndi nzeru yonse yeniyeni. 2 Wopusa sakondwera ndi kuzindikira; Koma kungobvumbulutsa za m’mtima mwace. 3 Pakudza wamphulupulu padzanso kunyoza; Manyazi natsagana ndi citonzo. 4…
1 Wosauka woyenda mwangwiro Aposa wokhetsa milomo ndi wopusa. 2 Kukhumba kosadziwa sikuli kwabwino; Ndipo wofulumira ndi mapazi ace amacimwa. 3 Utsiru wa munthu ukhotetsa njira yace; Mtima wace udandaula…
1 Vinyo acita ciphwete, cakumwa caukali cisokosa; Wosocera nazo alibe nzeru. 2 Kuopsya kwa mfumu ndiko kubangula kwa mkango; Womputa acimwira moyo wace wace. 3 Kuli ulemu kwa mwamuna kupewa…