Masalmo 71
Nkhalamba idziponya kwa Mulungu amene anamkhulupira kuyambira ubwana wace 1 Ndikhulupirira Inu, Yehova: Ndisacite manyazi nthawi zonse. 2 Ndikwatuleni m’cilungamo canu, ndi kundilanditsa: Ndicherereni khutu lanu ndi kundipulumutsa. 3 Mundikhalire…