Masalmo 131

Kudzicepetsa kwa Davide pakupemphera Nyimbo yokwerera, ya Davide. 1 Yehova, mtima wanga sunadzikuza Ndi maso anga sanakwezeka; Ndipo sindinatsata zazikuru, Kapena zodabwiza zondiposa. 2 Indedi, ndinalinganiza ndi kutontholetsa moyo wanga;…

Masalmo 132

Davide asamalira kacisi ndi likasa. Lonjezano la Mulungu Nyimbo yokwerera. 1 Yehova, kumbukilani Davide Kuzunzika kwace konse; 2 Kuti analumbira Yehova, Nawindira Wamphamvuyo wa Yakobo, ndi kuti, 3 Ngati ndidzalowa…

Masalmo 133

Cikondano ca abale ndi cokoma Nyimbo yokwerera; ya Davide. 1 Onani, nkokoma ndi kokondweretsa ndithu Kuti abale akhale pamodzi! 2 Ndiko ngati mafuta a mtengo wace pamutu, Akutsikira ku ndebvu,…

Masalmo 134

Afulumizidwa anthu kulemekeza Yehova Nyimbo vokwerera, 1 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse, Akuimirira m’nyumba ya Yehova usiku, 2 Kwezani manja anu ku malo oyera, Nimulemekeze Yehova. 3…

Masalmo 135

Mulungu alemekezedwa pa ukulu wace. Mafano ndi acabe 1 Haleluya; Lemekezani dzina la Yehova; Lemekezani inu atumiki a Yehova: 2 Inu akuimirira m’nyumba ya Yehova, M’mabwalo a nyumba ya Mulungu…

Masalmo 136

Mulungu alemekezedwe pa cifundo cace 1 Yamikani Yehova pakuti ndiye wabwino: Pakuti cifundo cace ncosatha. 2 Yamikani Mulungu wa milungu: Pakuti cifundo cace ncosatha. 3 Yamikani Mbuye wa ambuye: Pakuti…

Masalmo 137

Kudandaula kwa Ayuda ku Babulo 1 Ku mitsinje ya ku Babulo, Kumeneko tinakhala pansi, inde tinalira, Pokumbukila Ziyoni. 2 Pa msondodzi uli m’mwemo Tinapacika mazeze athu. 3 Popeza pamenepo akutigwirawo…

Masalmo 138

Davide ayamika Mulungu pa kukhulupirika kwace, naneneratu kuti mafumu onse adzatero Salmo la Davide. 1 Ndidzakuyamikani ndi mtima wangawonse; Ndidzayimba zakukulemekezani patsogolo pa milungu, 2 Ndidzagwadira kuloza ku Kacisi wanu…

Masalmo 139

Mulungu ali ponse ponse, adziwa zonse Kwa Mkulu wa Nsembe. Salmo la Davide. 1 Munandisanthula, Yehova, nimundidziwa. 2 Inumudziwakukhalakwangandi kuuka kwanga, Muzindikira lingaliro langa muli kutali. 3 Muyesa popita ine…

Masalmo 140

Davide apempha Mulungu amlanditse kwa mdani woipa wamphamvu Kwa Mkulu wa nsembe; Salmo la Davide. 1 Ndilanditseni, Yehova, kwa munthu woipa; Ndisungeni kwa munthu waciwawa; 2 Amene adzipanga zoipa mumtima…