Marko 11
Yesu alowa m’Yerusalemu alikukhala pa buru 1 Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, pa phiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ace, 2 nanena nao, Mukani,…
Yesu alowa m’Yerusalemu alikukhala pa buru 1 Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, pa phiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ace, 2 nanena nao, Mukani,…
Fanizo La osungira munda 1 Ndipo Iye anayamba kulankhula nao m’mafanizo. Munthu analima munda wamphesa, nauzunguniza ndi linga, nakumba moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina. 2…
Yesu aneneratu za masautso alinkudza 1 Ndipo pamene analikuturuka Iye m’Kacisi, mmodzi wa ophunzira ace ananena kwa Iye, Mphunzitsi, onani, miyala yotere ndi nyumba yotere. 2 Ndipo Yesu anati kwa…
Ansembe akulu acita ciwembu pa Yesu 1 Ndipo popita masiku awiri kuli phwando la Paskha ndi mikate yopanda cotupitsa; ndipo ansembe akuru ndi alembi anafunafuna momcitira ciwembu, ndi kumupha: 2…
Yesu aweruzidwa ndi Pilato 1 Ndipo pomwepo mamawa anakhala upo ansembe akuru, ndi akuru a anthu, ndi alembi, ndi akuru a milandu onse, namanga Yesu, namtenga, nampereka kwa Pilato. 2…
Yesu auka kwa akufa 1 Ndipo litapita Sabata, Maliya wa Magadala, ndi Maliya amace wa Yakobo, ndi Salome, anagula zonunkhira, kuti akadze kumdzoza Iye. 2 Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku…