Malaki 1
Kusayamika kwa Israyeli pa cikondi ca Mulungu 1 KATUNDU wa mau a Yehova wa kwa Israyeli mwa Malaki. 2 Ndakukondani, ati Yehova; koma inu mukuti, Mwatikonda motani? Esau si mkulu…
Kusayamika kwa Israyeli pa cikondi ca Mulungu 1 KATUNDU wa mau a Yehova wa kwa Israyeli mwa Malaki. 2 Ndakukondani, ati Yehova; koma inu mukuti, Mwatikonda motani? Esau si mkulu…
Mau akutsutsa ansembe 1 Ndipo tsono, ansembe inu, lamulo ili ndi la kwa inu. 2 Mukapanda kumvera, mukapanda kuliika mumtima mwanu, kupatsa dzina langa ulemerero, ati Yehova wa makamu, ndidzakutumizirani…
Za mthenga wokonzeratu njira ya Ambuye 1 Taonani, ndituma mthenga wanga, kuti akonzeretu njira pamaso panga; ndipo Ambuye amene mumfuna adzadza ku Kacisi wace modzidzimutsa; ndiye mthenga wa cipangano amene…
Oipa adzalangidwa, okoma adzadalitsidwa. Asamale cilamulo; adzafika Eliya 1 Pakuti taonani, likudza tsiku, lotentha ngati ng’anjo; ndipo onse akudzikuza ndi onse akucita coipa, adzakhala ngati ciputu; ndi tsiku lirinkudza lidzawayatsa,…