Luka 11
Pemphero la Ambuye 1 Ndipo kunali, pakukhala iye pamalo pena ndi kupemphera, m’mene analeka, wina wa ophunzira ace anati kwa iye, Ambuye, tiphunzitseni ife kupemphera, monganso Yohane anaphunzitsa ophunzira ace….
Pemphero la Ambuye 1 Ndipo kunali, pakukhala iye pamalo pena ndi kupemphera, m’mene analeka, wina wa ophunzira ace anati kwa iye, Ambuye, tiphunzitseni ife kupemphera, monganso Yohane anaphunzitsa ophunzira ace….
Yesu awacenjeza za cinyengo 1 Pomwepo pamene anthu a zikwi zikwi a khamu anasonkhana pamodzi, kotero kuti anapondana, iye anayamba kunena kwa ophunzira ace poyamba, Tacenierani nokha ndi cotupitsa mikate…
Maphedwe a Agalileya, tsanfa la Siloamu 1 Ndipo anakhalako nthawi yomweyo, anthu ena amene anamuuza iye za Agalileya, amene Pilato anasanganiza mwazi wao ndi nsembe zao. 2 Ndipo iye anayankha…
Yesu aciritsa munthu wodwala mbulu 1 Ndipo panali pamene iye analowa m’nyumba ya mmodzi wa akuru a Afarisi tsiku la Sabat a, kukadya, iwo analikumzonda iye. 2 Ndipo onani, panali…
Fanizo la nkhosa yosokera 1 Koma amisonkho onse ndi anthu ocimwa analikumyandikira kudzamva iye. 2 Ndipo Afarisi ndi alembi anadandaula nati, Uyu alandira anthu ocimwa, nadya nao. 3 Koma anati…
Fanizo la kapitao wonyenga 1 Ndipo iye ananenanso kwa ophunzira ace, Panali munthu mwini cuma, anali ndi kapitao wace; ndipo ameneyu ananenezedwa kwa iye kuti alikumwaza cuma cace. 2 Ndipo…
Za zolakwitsa, ndi makhululukidwe, ndi mphamvu ya cikhulupiriro ndi kutumikira kwathu 1 Ndipo anati kwa ophunzira ace, Sikutheka kuti zolakwitsa zisadze; koma tsoka iye amene adza nazo. 2 Kukolowekedwa mwala…
Fanizo la woweruza wosalungama 1 Ndipo anawanenera fanizo lakuti ayenera iwo kupemphera nthawi zonse, osafoka mtima; 2 nanena, M’mudzi mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu. 3 Ndipo m’mudzimo…
Zakeyu asandulika mtima 1 Ndipo analowa, napyola pa Yeriko. Ndipo taonani, mwamuna wochedwa dzina lace Zakeyu; 2 ndipo Iye anali mkulu wa amisonkho, nali wacuma. 3 Ndipo anafuna kuona Yesu…
Amfunsa Yesu za ulamuliro wace 1 Ndipo kunali lina la masiku awo m’mene iye analikuphunzitsa anthu m’Kacisi, ndi kulalikira Uthenga Wabwino, adamdzera ansembe akulu ndi alembi pamodzi ndi akulu; 2…