Habakuku 1
Cisalungamo ca Ayuda. Akasidi adzawadzera ndi kuononga zonse. Mneneri apempherera Ayuda 1 KATUNDU adamuona Habakuku 2 Yehova, ndidzapfuula mpaka liti osamva Inu? ndipfuulira kwa Inu za ciwawa, koma simupulumutsa. 3…
Cisalungamo ca Ayuda. Akasidi adzawadzera ndi kuononga zonse. Mneneri apempherera Ayuda 1 KATUNDU adamuona Habakuku 2 Yehova, ndidzapfuula mpaka liti osamva Inu? ndipfuulira kwa Inu za ciwawa, koma simupulumutsa. 3…
Akasidi omwe adzalangidwa 1 Ndidzaima pa dindiro langa ndi kudziika palinga, ndipo ndidzayang’anira ndione ngati adzanenanji mwa ine, ngatinso ndidzamyankha ciani pa coneneza canga. 2 Ndipo Yehova anandiyankha nati, Lembera…
Pemphero la Habakuku 1 Pemphero la Habakuku mneneri, pa Sigionoto. 2 Yehova, ndinamva mbiri yanu ndi mantha; Yehova, tsitsimutsani nchito yanu pakati pa zaka, Pakati pa zaka mudziwitse; Pa mkwiyo…